2019 sali pafupi kwenikweni koma ndale zija ndiye zafikapo basi. Pamene chipani chotsutsa cha Kongeresi chili pa kalikiliki otolela anthu, nawo a chipani cholamula cha DPP ayambapo kutsegula makomo awo. Dzulo lamulungu chipani cholamulachi chalandila… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Renowned Malawian musician Lucius Banda says he will contest against Atupele Muluzi at the convention of the United Democratic Front (UDF). Lucius Banda, who is also member of Parliament for Balaka North, said he is… ...
United Democratic Front (UDF) has turned the heat on Democratic Progressive Party (DPP) and President Peter Mutharika over plans to have Atupele Muluzi replace Saulos Chilima as DPP's running mate for the 2019 Malawi presidential… ...
Onse okonda nyerere ndi akufuna kwabwino, sonkhani limodzi limodzi kuti ulendo wa akatswiri a ligi opita ku CAF asauyende wapansi. Wa ana a Israeli mu chipululu. Ngakhale anakwela pachulu, kuziguguda pa chifuwa kuti iwo zivute… ...
Sanachiteko olo msonkhano umodzi oitanila anthu ku chipani. Olo kuvala makaka a chipani sanachiteko. Osewela mu timu ya Bullets amene tsopano walengeza kuti mtima wake uli pa ndale, Anong'a Fischer Kondowe wanena kuti iye ndi… ...
Bambo Francis Itende amene anatsomphola phasulo la a Mutharika agamulidwa kuti ndi olakwa. A Itende amene anachita chipongwe chawo chaka chatha pa 23 December anatsomphola phasulo m'manja mwa a Mutharika ati chifukwa amayesa muli ndalama.… ...
Eni ake akolawo ali ndi chimwemwe kuti akhwasula, kuti mavoti onse a Kum'mwera kwa mzinda wa Blantyre tsopano akhala awo. Koma kwa aneba awo ndiye kuli phwete. Pamene ndale zafika pa chi inde inde, chipani… ...
Democratic Progress Party (DPP) has warned Malawi Congress Party (MCP) to be wary of Reverend Maurice Munthali who joined MCP, saying the Reverend is unpredictable and behaves in the manner of a 'political prostitute'. DPP’s… ...
Tsopano mukakhala mmaluzi ndi kuganiza zoyamba bizimisi ya Tchalitchi muli muzichita uneneri, musamale. Azikumangani. A Polisi ku Thyolo anjata ndi kutengela ku Khoti Bambo Sampulo Newiri a utumiki otchedwa Thamanda ati kamba kofalitsa uthenga wa… ...
Ndi dzana lija nyimbo zinali zotamandila ndi zonyadilila akazi. Pano anthu ayamba kuimba za upandu ndi kuzitamandila pa uchigawenga. Nyimbo ina yopepela yautsa mapiri pa chigwa. Nyimboyi imene wayimba ndi mnyamata wina osadziwika kwenikweni otchedwa… ...
Uladi Mussa who was yesterday expelled from People’s Party (PP) says he will be joining another political party because he still has the steam in him. Uladi had claimed that PP was on the verge… ...
Dzukani Kwacha! Lekani kulota tsopano chifukwa DPP ikhala m’boma kudutsa 2019. Mlembi wa mkulu wa chipani cholamula cha DPP Mayi Greselder wa Jeffrey wanenetsa kuti mu zisankho za 2019 DPP ibubuda zipani zotsutsa. “Zoti DPP… ...
Patsepatse nkulanda. Kupalamula ndi konse ndithu koma milandu inayi ndendende kugenda ku Polisi wamkulu fodya ali mthumba. Bambo wina wa zaka makumi awiri ndi mphambu zisanu kudza imodzi (26) ali m'manja mwa a Polisi atagwidwa… ...
Kwatuluka tizithunzi ndipo tikufalitsidwa mu ma Fesibuku ndi mu ma WhatsApp umu. Mu Zithunzi zimenezi m’bambo wina wachikulire wapanilila ka msungwana mu mphechepeche kunyanja. Anthu akuti bamboyu ndi a Billy Gama amene ndi abusa a… ...
Ngakhale Atoti Manje anadandaula kuti pa galimoto zonse zili mdziko muno palibepo olo imodzi ya m’bale wawo, Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika wati a Malawi moyo wawo ukuyenda bwino kamba koti mu dziko… ...