The twists and turns of the road to 2019 have now started developing. Information that Malawi24 has indicates that the bromance between Peter Mutharika and Saulos Chilima is now approaching its final days as the… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Mmutu mwa phungu wa Kum'mwera kwa boma la Mulanje a Bon Kalindo otchuka kuti Winiko muli chilango chimodzi basi pa mlandu ulionse, kupha basi. Patapita nthawi a Kalindo atapempha boma kuti lizipha anthu onse okupha… ...
President Peter Mutharika has claimed that Malawians are happy with the roads his government is constructing across the country. He made the claim in Blantyre Wednesday during the ground-breaking ceremony of the bypass road from… ...
Musician Lucius Banda who rose to fame through criticism of vices among politicians especially stealing, is being accused of stealing as well. In a Facebook post that has gone viral, one Sam Smith Silumbu accuses… ...
…mpaka anabeleka ana awiri Zina ukamva, thupi lonse limagwidwa nyetsi. Munthu ndi mlongo wake amangidwa kwa chaka ndi theka zitadziwika kuti amazembelana mpaka kufika popatsana mimba kawiri ndi kubeleka ana. Malinga ndi nyuzipepala ina ya… ...
Just hours after President Peter Mutharika commissioned 55 megawatts of electricity from diesel powered generators, a section of Malawians have hit at the President. In a survey that Malawi24 conducted, residents of Blantyre lamented that… ...
Aiopela kutali. Olo asanaugunde mpira ndi komwe azitaya. Za CAF zija sanali maloto koma zilubwe. Pano mukamuona mzanu wa nyerere, musayambitse ya CAF mudana, ingokambani ya Super League. Masiku atangotsala pang'ono kuti nyerere zikaponde ku… ...
Reports reaching Malawi24 indicate that the CAF dream sold by Beforward Wanderers FC is on the verge of not materialising. According to the reports, the Nomads are trapped in so much trouble that has seen… ...
Abwelako ku Joni opanda kanthu. Angobwela ndi zovala zapathupi pawo ndi kaselula basi. Kaya ayambila pati kumudzi kuno? A Malawi okwana zana limodzi ndi theka kudza mphambu imodzi (151) afika m'dziko muno atathamangitsidwa ku South… ...
Mnyamata wina wa zaka 18 mu boma la Chikwawa amunjata atapha mzake ati polimbilana mkazi oyendayenda. Malinga ndi mneneri wa a Polisi mu bomali a Foster Benjamin, ati upanduwu udachitika pachinayi pamene abambo awiri amamwa… ...
Inu otsutsa, valani zilimbe chifukwa zoti mutenga boma 2019 ndiye ndi zosatheka, malinga ndi kafukufuku. Bungwe lina lochita za kafukufuku lati a Peter Mutharika ndi chipani chawo cha DPP akuoneka kuti ndiwo angawine chisankho cha… ...
Bwalo lalikulu la Milandu tsopano lamasula khonsolo ya mzinda wa Blantyre kuti ndi yololedwa kugwetsa nyumba zonse zomwe zamangidwa mu phiri. Khonsolo ya mu mzinda wa Blantyre inauza anthu onse omanga nyumba mu phiri kuti… ...
Zina ukamva kamba anga mwala ndithu. Pamene okuba mbuzi akutsekeledwa zaka, okuba galimoto akuchoka ku Khoti akusekelela. Bwalo la majisitileti ku Blantyre lagamula amuna awiri amene anaba galimoto kuti atsatsekeledwe. Ati m'malo mwake asachimwenso basi.… ...
Legendary musician and jazz trumpeter Hugh Masekela has died after a long battle with prostate cancer. He was 78. https://twitter.com/hughmasekela/status/955713727088775168 In a statement, his family said he had "passed peacefully" in Johannesburg "after a protracted… ...
Inatchuka nkhani yoti Wapolisi wa zachitetezo ananjatwa kamba kopita ku chimbudzi ku nyumba ya nduna zoona zophunzitsa anthu. Malinga ndi malipoti amene amagawidwa mma Facebook ndi WhatsApp, ati Wapolisi amene amapeleka chitetezo ku nyumba ya… ...