The secret dealings between the ruling Democratic Progressive Party (DPP) and the opposition People's Party (PP) will not last long and will not carry on to the 2019 polls. Former President Joyce Banda has announced… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Iran coach Carlos Queiroz believes Barcelona and Argentinean legend Lionel Messi is too good for a human being and has asked FIFA to investigate superstar striker if he is indeed human. Queiroz is so stunned by the… ...
Ululu wa Vita ukuzunguzabe Manoma. Mbwiza anavina Manoma ku Congo, Tchopa wa pa Bingu adakawazunguzabe a ku banja la nyerere. Inu, Vita si zibwana iyayi. Ndi izi lero Manoma ali ngati pa nsanja ya Babulo… ...
Wazitaya. Wazinyanyala. Wazidomoka. Wayendela yake. Wapita atanyangala ndipo walalika kuti a Chakwera ndi munthu wa nkhanza asananyamuke. Phungu wa dera lapakati mu boma la Salima a Felix Jumbe alengeza kuti tsopano alowa chipani cholamula cha… ...
A lawmaker from the main opposition CHADEMA party has been jailed in Tanzania for insulting President John Magufuli. The parliamentarian, Joseph Mbilinyi, has been convicted together with local leader for the party Emmanuel Masonga. According to a… ...
Ati kwawo kwatha. Ngati kuli kusolola, asolola basi ndipo amaliza. Tsopano ndi nthawi ya Kongeresi. A Sidik Mia amene analowa chipani cha Kongeresi auza anthu a DPP kuti alongeze katundu wawo mmboma chifukwa 2019 kulibe… ...
Nanthambwe wazitengela uku. Andione, andione wapezeka wakhalila zake zomwe. A Malawi aonetsa kukwiya ndi mfundo yomwe ananena Mayi Kabwila mu nyumba ya malamulo yoti boma lisiye kuzunza a Muluzi. Mu sabatayi Mayi Kabwila anaima mu… ...
President Peter Mutharika’s term is expiring in May. According to the electoral calendar that the Malawi Electoral Commission (MEC) has released, elections will be conducted on 21 May 2019 effectively signaling the end of Mutharika’s… ...
Death has been announced of the Malawian ambassador to the United Nations, His Excellency, Mr Necton Mhura. Ministry of Foreign Affairs and International Cooperation has confirmed Mhura's passing. However, there is no mention on the statement… ...
South Africa's embattled President Jacob Zuma has resigned, ending a 9-year rule seen by many as the most troubled period for the rainbow nation since the end of the apartheid. Zuma’s decision came after days of intense… ...
Death has been announced of veteran politician and former speaker, Sam Mpasu. A Facebook post by United Democratic Front (UDF) Ken Ndanga has announced that Mpasu passed on this morning at his home. Ndanga has… ...
Ena mutha kumapusitsana, ena kumanena nkhaniyi mutafunda bulangete, awonso atha kumainena monong’ona kuti ena asamve. Koma mphunzitsi wa Noma wangomasuka ndi kuima pachulu kukamba nkhaniyi. A Yasin Osman amene anatsogolera nyerere pa ulendo okakhomedwa ku… ...
South Africa's ruling African National Congress (ANC) has formally asked President Jacob Zuma to resign in the face of a corruption scandal that has sapped support for the party once led by Nelson Mandela. According… ...
Ndalama yokwana K72 miliyoni yasowa mu ofesi la bungwe loyang’anila za mayeso ndipo atafunsidwa munthu amene amayenela kuteteza, iye wati yasowetsa ndi njoka. Zochitika ku Africa ndi zodula mutu ndithu, zoopsa ndi zopatsa nthumanzi. Malipoti… ...
Manoma ametedwa mpala likuwala ku DR Congo pamene anzawo a Masters Security nawo angoti mwachaje satafuna, kubwela chimanjamanja ku Angola. Matimu onse awiri amene anakaimila dziko lino ku mpikisano wa CAF abwela chimanjamanja, osaona golo… ...