WhatsApp has crashed reportedly having been overwhelmed by 2018 New Year's best wishes messages. With the outage, the hashtag #whatsappdown is now trending on Twitter. WhatApp users in the Malawi took to social media to… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Apambana ligi, kawiri konse kufika mu ndime yotsiliza ya mipikisano ndipo akukamba zopita ku mpikisano wa CAF koma manoma ali ndi mthumba moyela.Maluzi ngati khoswe wa mu kachisi. Malinga ndi malipoti, akatswiri a ligi chaka… ...
A merry Christmas to you all. President Peter Mutharika and the First Lady have urged Malawians to emulate Jesus Christ during this festive period. The President and the First Lady have said this in a… ...
Enock Chihana has been reinstated as Alliance for Democracy (Aford) president. According to a consent order agreed by lawyers for Chihana and Aford members who obtained an injunction against him, even though his term expired… ...
Msogoleri wa chipani cha Kongolesi, m'busa Lazarus Chakwera, wasambwadza Pulezideti wa dziko lino, Pulofesa Peter Mutharika, kuti asiye kuloto zoti n'kudzapambana pa chisankho chapatatu chomwe chichitike mu chaka cha 2019. M'busa Chakwera audza a Mutharika… ...
Urban musician Ritaa has caught the ire of some Malawians on social media for what they term is her ‘indecent’ dressing. In a Facebook post that was promoting her song, Winner, a section of Malawians… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika ati anthu azipani zotsutsa ndi amabungwe amafuna kusintha malamulo ochitila chisankho cholinga choti amuchotse pa udindo. A Mutharika adanena izi lachiwiri pamene amayika mwala wa maziko pamalo amene… ...
Phungu wa dera la pakati mu boma la Lilongwe a David Bisnowaty aputa mavunkhomola. A Bisnowaty dzulo lolemba anajambulitsa ndi Mafumu a mu dera lawo ati atatchena ma suti amene Phungu'yo wawagulila. Polemba pa tsamba… ...
... MP says it was a campaign promise The decision by Lilongwe City Centre MP David Bisnowaty to donate suits to Chiefs in his area has only pleased himself and the Chiefs. Comments on social… ...
Wakwiya ndi mfiti. Amene sakusangalala pano ndiye mwina ndi neba basi. Kuli chisangalalo ku banja la nyerere. Ku manoma lero amwa wamkaka, kusamba wa mkaka ndipo chilichonse kwa iwo chili tayale. Patatha zaka khumi ndi… ...
A suit by musician and pastor Mlaka Maliro has become a Facebook sensation in Malawi. In viral photos, Pastor Mlaka Maliro of the Enlightened Gathering Church whose leader is Shepherd Bushiri can be seen in… ...
…chipani cha DPP chikhumudwa nawo Wachiwili kwa Mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima anauza a Malawi kuti apite ku zionetselo pa 13 December chaka chino. A Chilima ananena izi mu mpingo wa katolika ku… ...
Alliance For Democracy (AFORD) deputy district governor for Rumphi Newton Harawa has been severely beaten by unknown thugs. According to sources within AFORD, Harawa has been beaten by thugs at his house in Rumphi. Thugs… ...
Africa Confidential, one of Africa's celebrated publications, has described as a 'pact with the devil' the alliance that former Malawi president Joyce Banda is forging with the ruling Democratic Progressive Party (DPP). According to reports… ...
Karonga Central Member of Parliament (MP) Frank Mwenifumbo has pleaded with Malawi to consider legalising prostitution, claiming a lot of people in the country rely on the sex trade. “We see young ladies and young men standing… ...