… Chifukwa walabvulira mzake Wadyanso wani Gabadinho Mhango mu dziko la South Africa. Ambiri akukamba za iye. Koma m'malo momuyamikila kuti ali ndi luso logometsa mafuko pokankha chikopa, anthu akuti khalidwe la Gaba ndi lonunkha… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
November promises to be a good month for Malawians and Chaponda. Comedian Daliso Chaponda will be in the country in November where he will entertain comedy lovers in the city of Blantyre before moving to… ...
Nawo ndi a Malawi ndipo atopa ndi zotsalidwa. Tsopano akupempha kuti boma liwathandize kuti nawo azimva kuti ndi mzika za dziko lino. Amayi oyendayenda auza boma kuti lisiye kuwayang’anila pansi ndi kuwathandiza kuti nawo azikhala… ...
The triumphant entry into Blantyre by the Carlsberg cup champions, Big Bullets has seen the death of one person. According to information, a Malawi under 16 player lost his life in joining the people's team… ...
Four people were arrested yesterday after the match at Bingu National Stadium accused of stoning the Nomads bus and players. According to information that Malawi24 has, after defeating their rivals in the finals of the… ...
Awatibulanso. Kachikena awatsambitsa madzi a matope. Ku Bingu anapita akusangalala kuja, Manoma atuluka ndi nkhope zozyolika akulila mayomayo. Pa masewero amene anakodola khamu, maule lero aliritsa nyerere kachikena atazitsomphola chikho cha Carlsberg. Anali masewero oyamba… ...
Nyau ina mu boma la Mchinji ikuonela pakhosi anthu ena okwiya ataitsina ndi makofi olapitsa. Malinga ndi malipoti, pa tsikulo panali mwambo oveka ufumu wa a gulupu aakulu a Magombo mu dera la mfumu yaikulu… ...
Just a day after announcing a bloodless coup on the leadership of Joyce Banda over the dysfunctional opposition People's Party (PP), Uladi Mussa has courted trouble. A People’s Party member loyal to former President Joyce… ...
...JB has no mandate over PP, says Uladi Mussa Things have fallen apart in People's Party where Uladi Mussa, the party's acting president, has said he no longer recognises Joyce Banda as PP's president. Change… ...
A Roman Catholic priest serving Balaka Parish was found dead on Wednesday. According to the Catholic Secretariat of the Episcopal Conference of Malawi (ECM), Reverend Father Callisto Baluwa of the Society of Montfort Missionaries was… ...
A ku unduna woona za chilengedwe, mphamvu ndi migodi ati iwo satopa kulimbana ndi anthu onse amene ali pa kalikiliki kufukula mchenga. Malinga ndi a Sangwani Phiri amene amayankhulila undunawu, iwo ati undunawu ndi okhumudwa… ...
The Supreme Court in Kenya has annulled the result of the last month's presidential election. Citing irregularities, Chief Justice David Maraga said a new vote should be held within 60 days. Justice Maraga said the… ...
He promised it and he has delivered it. President of the so-called United States of Mulanje and Thyolo Vincent Wandale has introduced his cabinet. In a Facebook post, Wandale threw a picture of him and… ...
Mtsogoleri wa zipani zotsutsa mu nyumba ya malamulo amenenso ndi otsogolera chipani cha Kongeresi wanenela a Mutharika ndi chipani chawo cha DPP kwa azungu. Mu chikalata chimene a Chakwera alembela a kazembe a mayiko a… ...
Posachedwapa pofuna kukaona phiri ku Mulanje kapena kujambulitsila mu tiyi ku Thyolo, a Malawi tizifunika kupita ndi chiphaso choyendela (passport). A Vincent Wandale amene adalengeza kuti maboma a Thyolo ndi Mulanje ndi dziko loima palokha,… ...