Ngakhale a bungwe loona za madzi mu Lilongwe la Lilongwe Water Board linanena kuti madzi a ku Area 18 atha kumwedwa tsopano, nduna ya zofalitsa nkhani a Nicolas Dausi ati iwo sangamwe madzi otuluka ku… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Mapeto a sabata awa anali okoma kwambiri kwa nyerere. Atagonjetsa timu ya Moyale pachiwelu, dzulo anaswanso khofi kwa ana asukulu a Mzuni pakwawo pomwe. Pa masewero amene anachitika pa Mzuzu stadium a mpikisano wa ligi,… ...
South African revolutionary politician Julius Malema has denied claims by the pressure group Transformation Alliance that he was lined up to speak in Malawi this weekend. Malema who leads the revolutionary Economic Freedom Fighters (EFF)… ...
Anthu onse ogwila ntchito mmboma ayembekezela kukokana ndi ma landilodi mwezi uno chifukwa boma lalengeza kuti malipilo awo alandila pa 45. Malinga ndi chikalata chimene chalembedwa ndi a unduna wa zachuma ndipo chasayinilidwa ndi a… ...
Anthu ena akudabwa kuti anali aakulu ngati n’gombe mwina kapena ochepa koma msinkhu wa mphaka kapena mwana wa khanda. Mtsogoleri wa dziko la Nigeria a Muhammadu Buhari alengeza kuti sazipita ku ofesi yawo ati chifukwa… ...
Bambo Edgar Kulemeka amene pa 11 mwezi uno anabaya Mayi Sally Mkwezalamba pofuna kuthawa ngongole anjatidwa tsopano. Malinga ndi Apolisi, achibale a Kulemeka ndiwo anakatula mkuluyo ku Polisi patatha sabata akuyenda chothawathawa. A Kulemeka ati… ...
Kunali kanthu ku Balaka pamene chipani chotsutsa cha Kongeresi chinachititsa msonkhano pa sukulu ya Balaka Primary. Msonkhanowu umene unasonkhanitsa akuluakulu a chipanichi kuphatikizapo a Sidik Mia unakodola khamu loti a Kongeresi sanalionepo ku chigawo cha… ...
Muthokoze kuti mabwana anu alibe nazo ntchito ndipo boma la Malawi sililabadila zotelezi koma enanu bwenzi mutaimitsidwa pa ntchito kamba kosavala thayo. Ogwila ntchito ena a mmboma mu dziko la Uganda aimitsidwa pa ntchito kwa… ...
Suspended Times talkshow host Brian Banda has disclosed that he has been suspended from the institution for not hitting at the ruling Democratic Progressive Party (DPP) harder in his programming. In a leaked audio Banda… ...
Trouble is brewing at the oldest news publishers in Malawi, leaked audio conversations have revealed. According to viral audios that have revealed the rot at Times Group Limited which owns Times Radio and Television, two… ...
Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF), a Atupele Muluzi ati iwo sanapinyolitse chipanichi kwa a Mutharika. A Muluzi amene ndi nduna mu boma la a Mutharika anauza anthu ku Ndirande kuti iwo ndi… ...
Samalani oyendetsa minibus chifukwa ngakhale nduna tsopano zalowelela pa nkhani yolanga anthu onse ochita chibwana ndi malamulo a pamseu. Nduna yoona za m’dziko a Grace Obama Chiumia anadabwitsa anthu mu mzinda wa Mzuzu pamene analanda… ...
Kenya Election: President Uhuru Kenyatta of Kenya has been declared winner of the polls the country had on the 8th. An official announcement from the country's electoral management body, the IEBC, has declared Uhuru as… ...
…Parliament failed to account for over K11million used on prepaid airtime units An audit report by the Malawi Auditor General on the government accounts offers a chilling account of the financial management system that has… ...
An audit inspection of the financial records of the Office of the Vice President has revealed K196 million cashgate at the Office of the Malawi Vice President, Saulos Chilima. “An examination of payment vouchers and… ...