Kuwonjezera kwa ndalama zachitukuko za Constituency Development Fund (CDF) kuchoka pa 100 miliyoni kufika pa 200 million kwacha kunadzetsa chimwemwe chochuluka kwa aphungu ambili pamene nduna ya za chuma a Simplex Chithyola Banda anawuza nyumba… ...
Articles By Ben Bongololo
Bambo wazaka 50 a Chiyipila Nsato, ali m'manja mwa apolisi ku Lilongwe kaamba kowaganizira kuti iwo ndi anthu ena atatu anakaba nawo katundu okwana 90 miliyoni kwacha ku likulu la tsopano la Radio Maria. Mneneri… ...
Njonda ina yazaka 30 zakubadwa, yapulumukira mkamwa mwa njovu pamene bwalo lamilandu ku Kasungu lamupeza osalakwa pa mlandu omwe amamuzenga ogonana ndi mtsikana yemwe amati ndi wa zaka 16. Mkuluyu yemwe dzina lake ndi Lameck… ...
Apolisi ya Nkhunga m'boma la Nkhotakota, akusakasaka dalayivala wina yemwe ananyamula chamba cha nkhaninkhani mu galimoto yomwe iye amayendetsa ndipo atazindikira kuti apolisi akumutsatira anayimika galimotoyo pa malo ena mkuliyatsa liwiro la mtondo odooka. Nkhani… ...
Malingana ndi kukwera kwa zinthu zosiyanasiyana mdziko muno, nayo kampani ya Nacala Logistics yalengeza kuti yakweza mitengo yonyamulira anthu pa sitima ndipo mitengo yatsopanoyi iyamba kugwira ntchito pa 1 March chaka chino cha 2024. Kampaniyi… ...
Apolisi ku Limbe mumzinda wa Blantyre akusunga mchitokosi bambo wina wa zaka 34 pamene iye ndi azake ena anayi anachitira chiwembu munthu wina woyendetsa njinga yamoto yakabaza ya mtundu wa Lifan LF 150-7 yomwe nambala… ...
Anthu awili afa ndipo ena avulala pangozi yagalimoto yomwe yachitika lero pamudzi wa Machinga m'boma la Dowa mu nsewu wa Salima-Lilongwe pamene galimoto yomwe anakwera inalephera kukwera chitunda zomwe zinapangitsa kuti ibwelele m'mbuyo mpaka kukagwera… ...
Anthu okhala m'boma la Karonga m'mudzi mwa Mwangosi mfumu yayikulu Kilipula ayamba kuthilira mbewu zawo m'minda yawo pamene kwakhala pafupifupi masabata atatu kopanda mvula. Nelson Manda yemwe ndi ophunzira wapa sukulu ya ukachenjede ya Mzuzu… ...
Bambo wina wa zaka 32 zakubadwa akusungidwa mchitokosi cha apolisi ku Monkey-Bay m'boma la Mangochi kaamba komuganizira kuti wakhala akugwililira mwana wake wa zaka 12 mpaka kufika pomupatsa mimba. Alice Sichali yemwe ndi mneneri pa… ...
Prophet Shepherd Bushiri yemwe ndi mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering (ECG) walengeza kuti wayamba pologalamu yogawa chimanga kwa maanja oposa 1 miliyoni omwe akhudzidwa ndi njala mdziko muno. Malingana ndi a Bushiri omwe… ...
Katswiri pa nkhani za ndale m'dziko muno a Lyford Chadza, walangiza Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera ponena kuti uthenga wake wa SONA ukhale opereka chiyembekezo poona nyenyo zomwe dziko lino likudutsamo. Katswiriyu wanena… ...
Sukulu ya ukachenjede ya Mzuzu yalengeza kuti ophunzira omwe akupitiliza maphunzilo pasukuluyi adzayamba maphunzilo awo amchigawo choyamba lolemba pa 19 February 2024 m'malo mwa pa 12 February. Kudzera mchikalata chomwe Malawi24 yaona, sukuluyi ikudziwitsa anthu… ...
Kutsatira ulosi omwe nthambi yoona za nyengo mdziko muno inachita ponena kuti mvula iyamba kugwa pa 1 February mwezi uno, tsopano a Malawi ambili ayamikila ulosi wanthambiyi pamene mvula yagwadi m'madera ochuluka ngati momwe nthambiyi… ...
Apolisi ku Mulanje anjata njonda ziwiri zomwe zakhala zikuzinganiziridwa kuti zakhala zikuchita za umbanda mbomali. Mneneri wa apolisi ku Mulanje a Innocent Moses watsimikiza za nkhaniyi ndipo iye wati njonda ziwiri mayina awo ndi a… ...
M'modzi mwa akatswiri pandale mdziko muno wachenjeza a Kondwani Nankhumwa kuti akuyenera kupanga chiganizo mosamala pa zatsogolo lawo pandale ponena kuti akapanda kusamala atha kudzikumbira okha dzenje lomwe iwo sangathe kutulukamo. Malingana ndi Katswiriyu, a… ...