Mpungwepungwe unakula m'nyumba ya malamulo pamene mbali ya boma yavomereza lamulo kuti ulimi wachamba udzilimidwa m'dziko muno. Izi zinadzetsa mpungwepungwe kunyumbayi pamene aphungu achipani chotsutsa cha Democratic Progressive Party (DPP) anati sakugwirizana ndi lamuloli. Izi… ...
Articles By Ben Bongololo
Anyamata awiri akusungidwa mchitokosi cha apolisi ku Mwanza atagwidwa ndi bomba pa malo ochitira chipikisheni munsewu wa Mwanza-Blantyre pomwe iwo anali pa ulendo wawo okalithira nsika bombali. A Hope Kasakula yemwe ndi wofalitsa nkhani pa… ...
Nduna yoona za chuma mdziko muno a Simplex Chithyola Banda walengeza za kukwera kwa ngongole yomwe ophunzira a msukulu za ukachenjede amalandira kuchoka pa K350, 000 pachaka kufika pa K560,000. A Chithyola Banda anena izi… ...
Mdima wagwanso m'dziko la Nigeria pamene katakwe opanga mafilimu yemwe dzina lake ndi Amaechi Mounagor wadziwika kuti wamwalira atadwala nthenda ya impso. Izi zikudza pasanathe mwezi dzikoli litatayanso katswiri wina a John Okafor yemwe amadziwika… ...
M'modzi mwa anthu omwe amayankhulapo pazochitika m'dziko muno Lyford Chadza wapempha alangizi a mtsogoleri wa dziko lino kuti adzimuwunikira mtsogoleriyu mwatchutchutchu ponena kuti a Chakwera achedwa kulengeza kuti m'dziko muno muli njala. A Chadza ati… ...
Bungwe loona za ufulu wa anthu mdziko muno la Malawi Human Rights Resource Centre (MHRRC) lati dziko la Malawi likuyenera kusintha mwa zina zomwe zimalepheletsa atsikana ndi amayi kupeza nawo thandizo lochotsa pakati motetezedwa. A… ...
Bwalo la milandu ku Lilongwe lalamula a Arafat Goman kukakhala kundende kwa zaka 63 pa mlandu wakupha a Cecilia Lucy Kadzamira azaka 82 amene adali mchemwali wa a Tamandani Kadzamira, mthandizi wa mtsogoleri wakale wadziko… ...
M'busa wa mpingo wa Bua African Abraham ali m'chitokosi cha apolisi ku Mchinji kaamba koganizilidwa kuti adaba mawaya amagetsi wa ndalama zokwana K297,000 a bungwe lopereka magetsi la Escom. Mneneri wa apolisi m'bomali watsimikiza zankhaniyi… ...
Bambo wina wazaka 49 wa m’mudzi mwa Binya kwa mfumu yaikulu Kwataine ku Ntcheu, watsikira kulichete atamwa matoti 42 akachasu pampikisano wazidakwa opapira bibida omwe unachitika dzulo mbomali. Nkhani yonse ikuti dzulo lolemba pa 11… ...
Fostina Mbemba ndi amene wathamanga kuposa atsikana anzake mu mpikisano wa Mzuzu City Half Marathon lero. Mtsikanayu analibutsa liwiro ngati kulibe mawa ndipo iye anathamanga mtunda okwana 21 kilomitazi pa ola limodzi ndi mphindi zokwana… ...
Chikondi Mwanyali ndi amene wapambana masewera a Mzuzu City Half Marathon atathamanga mtunda otalika makilomita okwana 21 pa ola imodzi ndi mphindi zokwana zisanu ndi chimodzi. Mkulu wina amenenso wakonkhomola lekodi ndi Chancy Master pamene… ...
Zachitikanso lero mumpingo wakatolika ku Lunzu pamene wansembe wathira bakera kukamwa oyambitsa kwaya kamba koyambitsa nyimbo ya Aleluya mu nyengo ino ya lenti mpaka mapemphero kusokonekera. Nkhani yonse ikuti a Edward omwe ndi oyambitsa kwaya… ...
Mpikisano othamanga wa Mzuzu City Half Marathon wayambika pamene ma athletes ayamba kuthamanga mtunda okwana 21 kilometres kuchokera pa St John's munzinda wa Mzuzu. Kuno kuli liwiro lamtondo wadooka pamene anyamata komanso asungwana akulikumba liwiro… ...
Kunali kusinthana zibagera mkachisi wa Zolozolo CCAP yomwe uli pansi pa Livingstonia Synod ku Mzuzu kamba ka mkangano omwe unabuka pankhani wokhudza zachuma pakati pamamembala ndi akuluakulu ena ampingowu mpaka apolisi anathira utsi okhetsa misonzi… ...
Adzukulu okumba manda amangilira anthu awili pamtengo kumanda a Kabwabwa kamba kotolera chipepeso cha maliro popanda chilolezo kuchokera kwa amfumu a ku Area 25B (Kabwabwa) munzinda wa Lilongwe. Mayina a anthu awili omwe amangidwa pamtengowa… ...