M'tsogoleri wakale wa dziko la Zambia, a Edgar Chagwa Lungu, wati zitengera a Malawi kukavotera m'tsogoleri amene ndi wongoyeselera zinthu kapena wodziwa zinthu, maka pachisankho chomwe chichitike chaka chamawa m'dziko muno. A Lungu ayankhula izi… ...
Articles By Ben Bongololo
Meet Tabitha Chawinga, a young woman from Malawi who has made history by becoming the first woman to win France's National Professional Footballers Player-of-the-Year Award in the women's category, joining the likes of Kylian Mbappe… ...
Patangodutsa sabata imodzi pomwe Prophet Shepherd Bushiri adapeleka ndalama zokwana 6 miliyoni kwacha kwa 'M'neneri' Habakkuk kutsatira pempho lomwe adapereka, lero Habakkuk wapemphanso thandizo lina kwa m'neneli Bushiri. Mneneri Habakuk ati akufuna thandizo loti amangire… ...
Ayi ndithu lero mu Tnm Super League zavutirapo ndithu pamene imodzi yokha ndiyo yaluza pamene ena anayi afanana mphamvu pakutha kwa masewero lero pa 11 May 2024. Mighty Mukuru Wanderers yamwa mkaka wa ngambwingambwi pomwe… ...
Sukula ya sekondale ya Msiki m'boma la Mzimba ikusimba lokoma potsatira thandizo lokwanira 4.3 miliyoni lomwe lalandira kuchokera kwa ophunzira akale pa sukulu yaukachenjede ya Mzuzu. Masiku anayi apitawo, ophunzira akale pa Mzuzu University anadzidzimutsa… ...
Kunali kumwemwetera chakumasanaku ku Dedza pamene timu ya Dedza Dynamos yatembenuza chikwangwani nkukhala Premier Bet Dynamos kutsatira mgwilizano omwe timuyi yasayinira ndi kampani ya Premier Bet wandalama zokwana 100 miliyoni kwacha. Kampaniyi yati iziperekanso ndalama… ...
M'nyamata wina amene wakhala akunamizira kuti ndi ophunzira pasukulu ya Ukachenjede ya Mzuzu ali mu uluru osaneneka kutsatira kumenyedwa ndi ophunzira pasukukuyi pomuganizira kuti anaba mafoni awiri awophunzira ena. Amon Chimalawalana, yemwe watiuza nkhaniyi, wati… ...
Kunali mkoke mkoke lero mu Tnm Super League pamene anyamata amakudzulana nthenga, kugwalulana zibwano, kuchotsana chimbenene. Uyu ndi tsatanetsane wamomwe lero masewero athera. Mighty Wanderers yalepherana ndi timu ya Bangwe All Stars, ndipo masewero athera… ...
Mtsogoleri wadziko lino a Lazarus Chakwera lero anyamuka kupita mdziko la Kenya komwe akakhale nawo pa msonkhano wa banki yayikulu yadziko lonse ya World Bank. Mtsogoleriyu akuyembekezeka kudzanyamuka kudzera pabwalo la ndege la Kamuzu munzinda… ...
Mtengo wautali salozerana ndipo nyimbo yomwe yadya nambala one pa YouTube ndi ija ya mkulu odikula uku akutudzula mbina maka ikafika paja akumati "She got me feeling like ah ah ah ah ah ah!" Tsopano… ...
The Malawi Bureau Standards (MBS) has taken swift action, suspending restaurant operations at Hotel Victoria's and Heritage Hotel by Serindib in Blantyre due to hygiene violations. According to MBS, the immediate suspension of the restaurant… ...
HIV law has remained unknown to many since its introduction in 2018. The National AIDS Commission (NAC) is raising the alarm that a large part of the population is unaware of the HIV and AIDS… ...
Kwachema kwa Manase ku Blantyre pamene apolisi ayamba kunjata anthu onse omwe akugulitsa mowa omwe ndi owopsa ndipo ukutchulidwa ndi mayina monga: Ambuye tengeni, magaga, komanso taya njinga omwe pakadali pano waphapo anthu asanu (5).… ...
Ofesi ya Zaumoyo m'boma la Blantyre yati ikufufuza za imfa ya anthu asanu omwe amwalira kutsatira atamwa mowa osadziwika bwino ndipo ofesiyi yati idzabweretsa poyera zotsatira zakafukufuku-yi akatha. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe khonsolo… ...
Ophunzira wamkazi wa sitandade 5 ku Mulanje wadzipha chifukwa chokwiya ndi malangizo amayi ake omuletsa khalidwe lake lopanga zibwenzi atadziwa kuti akuchita chibwezi ndi m’nyamata wina mdelaro. Nkhani yonse ikuti mtsikanayu, yemwe dzina lake ndi… ...