Wamasuka tsopano m’busa Brown Mpinganjira. Wayambapo zija zokhuthula mawu pa misonkhano yandale. Nkhani pano si ya PP anaisiya ija koma ya DPP. Ndipo iye wachenjeza anthu a kummwera kuti asazayese kuvotela Kongeresi. Amene anali wachiwiri… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Anthu awiri amene amatsogolera anzawo pochitila mtudzu President ndi kumema anthu kuti achite zionetselo anjatwa. Izi zachitika mu dziko la Tanzania limene Mtsogoleri wawo John Magufuli wayamba kuonetsa makhalidwe achilendo ofuna kupondeleza ufulu wa anthu.… ...
Deputy Inspector General (DIG) of Police responsible for administration Duncan Mwapasa is expected to be appointed Inspector General of Police to replace According to reports, Kachama is supposed to retire in May this year and… ...
Forget all the rhetoric of beating Chakwera in the 2019 polls and holding on to the Presidency until 2024, this is President Peter Mutharika’s last term. According to a self proclaimed man of God who… ...
Cashgate convict Leonard Kalonga has been handed a 7-year jail sentence for stealing close to K4 billion of public funds. Kalonga, who worked as Ministry of Tourism Assistant Director, was convicted in August 2015 for his involvement… ...
Bukhu loyera Mateyu 22 vesi la 21 Akhristu ambiri akulidziwa ndipo akuyenela kuchita umo linenela. M'busa otchuka mu mzinda wa Blantyre, a Joseph Ziba amangidwa ati kamba kothawa kupeleka msonkho okwana 26 miliyoni Kwacha. Malinga… ...
Supreme court grants bail to cashgate suspect, Ralph Kasambara, pending an appeal of his conviction. Former minister of justice Ralph Kasambara was handed a 13 year jail sentence in August 2016 on the count of… ...
The immediate family of slain Malawi cabinet minister Dick Matenje has accused Malawi Congress Party (MCP) of playing cheap politics by misleading the nation that the family has joined the party. Richard Dick Matenje, a… ...
Former Malawi cabinet minister, Patricia Kaliati, has lost over one million Kwacha to a fraudster who has conned several DPP and government officials. According to published reports, Kaliati deposited the money into an Airtel Money… ...
Ati a Mutharika ndi chipani chawo cha Democratic Progressive (DPP) agwilira dziko lino. Aliveka manyazi. Kuliyamwa kalikonse ndi kulisiya mbu. Lokhuta ndi umphawi. Koma a Malawi musadandaule, chifukwa ati a Chakwera ndi chipani chawo cha… ...
A 5.6 magnitude earthquake has hit Nsanje district. The tremor, reportedly the strongest since the sequence of earthquakes that struck Karonga district in 2009, lasted for about 10 seconds. According to information published by U.S.… ...
Kodi mwaona kale kuti nyumba zanu ndi zodalilika? Ndiye kuli zimbudzi, zija zimangogwa ndi Mvula, munamanga zolimba? Bungwe loona za nyengo mu dziko muno lanena kuti a Malawi akhale okonzeka chifukwa Mvula ya mphamvu ikuyembekezeleka… ...
Nkutheka kuti inu simunamwepo koma mwina azanu munakhisana nawo aja anamwapo. Madzi atubvi la khatikhati anavuta ku Lilongwe aja atulukiranso. Pano ndiye adza ndi ukali, kununkha kwakeko ndiye ngati wangowatunga mu suweji madziwa kuti umwe.… ...
Pa ngodya zitatu za chipani cholamula cha DPP chija, imodzi ndiye ikukhala ngati ikuvutilapo. Anthu akugonabe ndi mantha, Chitetezo ndi kumpanda wachifumu kokha basi. Anthu a mmudzi mwa Goma m’boma la Chikhwawa akukhala mwa mantha… ...
A PP kodi mulipo? Pitani ku maofesi a chipani chanu chifukwa Mtsogoleri wanu ati akubwera ndipo 2019 akhala akupikisana nawo pa chisankho. Malinga ndi malipoti a olemba nkhani, Mayi Banda alengeza zoti azapikisana nawo pa… ...