Wazitaya. Wazinyanyala. Wazidomoka. Wayendela yake. Wapita atanyangala ndipo walalika kuti a Chakwera ndi munthu wa nkhanza asananyamuke.
Phungu wa dera lapakati mu boma la Salima a Felix Jumbe alengeza kuti tsopano alowa chipani cholamula cha DPP.

A Jumbe alengeza izi kudzela pa tsamba lawo la Facebook kuti tsopano iwo ndi a chipani cholamula ndipo mu 2019, iwo akuima ngati wa DPP.
A Jumbe anenanso kuti iwo sazaimanso ku dera lawo lapano, ati m’malo mwake akukayima ku dera la kumpoto mu boma la Salima lomwelo komwe kuli kwa Mayi awo.
Atauzidwa kuti iwo akagonja kumene akupitako kamba koti DPP ilibe chikoka, a Jumbe adanena kuti anthu ndiwo awatuma.
A Jumbe adachotsedwa mu chipani cha Kongeresi mu chaka cha 2016.
Ngakhale adatenga chiletso ku bwalo la milandu, a Jumbe ndi Kongeresi akhalila kulumana.
172 thoughts on “Nkhanza za Chakwera zandipititsa ku DPP – Jumbe”
Comments are closed.

minister of agriculture 2019 mr jumbe welcm mu dpp
now u have really shown us why u were doing that to our mighty MCP . Unatumidwa ndi DPP
Anali kare wa dpp ameyo asatipusise
Kkkkkk chipinda cha MCP kuli kanthu
Takulandilani ku DPP Mr jumbe nkhalani omasuka ndithu.
Amudyetsa Chi #Banzi, Sakufuna Cash Gate Imuphonye.
Ndikanakonda Ma Comment Awa Aziwerenga Nawo Anthu Ngati #jumbe.
KKKKKK KAYA MR J
Salima Central tizavotera Jerald wa MCP
End of his journey in politics
Nansongole owonekeratu sitimamusiya kunzulilatu pompopompo man. Musiyeni spite gurokunyindayo
Takulandilani inu munthu wabwino bwino mumafuna muyipe chifukwa cha anthu ena eti
Ma tractor mudaba aja bwana, muzalowa ndithu
Iyaaaaa dyera lanu akulu nusatinamize apa anthu ngati inu mukuononga dziko
MORE FIRE JUMBE NO BACK MCP
What agood and mature decision you have made.Ndipemphe anzanga aDPP.Mulandileni ndi mtima onse nzanuyo.He is intelligent young man.He can help the party do good things in addition to what you are already doing.I don’t hate MCP.Its where we are all coming from but we need true representation in the party .Not power on type of leadership but power to.Muwuzeni Dr. Kabwila aganize bwino naye.Tikusowa nzeru zake kuyendetsa dziko.Akapusa akhala garu wa Mbusa Chakwera.Uladi Mussa;You are intelligent make a quick decision before its too late.Late make Salima home of peace and wise politician.Ndakulila mu MCP ndikudziwa chomwe ndikunena.Ndinakhala Earial Treasure ndili Std8.Iwas forced to and Idid what they asked me to.I love the party (MCP) except what I see and hear.Good lucky Jumbe.
Wasala uyu uyu amapha Ng’ombe kumakatayu nayeso abwela ekhaa