Just days after the CCAP Nkhoma synod issued a Pastoral letter, the Catholic Church in Malawi has issued their own. The letter which has been read in all Catholic Parishes in Malawi this morning has,… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Ngati muli akuluakulu a bungwe lija la Sulom, ati chonde lero zipumi zanu zisaoneke ku Bingu National Stadium kumene maule apalane mamba ndi nyerere. Malinga ndi chikalata chimene a Malawi24 anapatsidwa chosayinilidwa ndi mkulu wa… ...
Kaya muli chani m’chuinomu choti mpaka ndi kufika poimitsa maphunziro kenako sukulu ndi kutsekedwa ndithu? Ma lipoti amene Malawi24 yalandila aonetsa kuti sukulu ya za ulimi ya Mwimba ayamba aitseka kaye. Ati akulu akulu a… ...
Nkhani ija ya ndege ija, zija anamutchula a Lutepo zija, mwinanso zija adanena a Kasambara zija. Mneneri wa a Polisi mu dziko muno a James Kadadzera ati chilolezo chomwe a Polisi adatenga chowapatsa mphamvu yonjata… ...
Kwanuko akukamba ya ndani? Kunotu anthu nkhani ndi ya Amayi. Atakhala kunja kwa dziko lino kwa zaka pafupifupi zinayi, Mtsogoleri wa kale wa dziko lino Mayi Joyce Banda ati akubwera. Malinga ndi chikalata chimene atulutsa… ...
Inkosi ya Makosi Mmbelwa, imene ndi Mfumu yaikulu ya Angoni, yadzudzula a Livingstonia Synod ndi kuwachenjeza kuti akapanda kusamala athamangitsidwa mu dera lake. Pa mwambo oveka ufumu a T/A Mzukuzuku ku Mzimba, mlembi wamkulu wa… ...
Mpingo wa Katolika mu Diocese ya Zomba watulutsa chikalata choonetsa kukhumudwa ndi wansembe wawo a Thomas Muhosha amene anamangidwa poganizilidwa kuti anatengapo mbali pa imfa ya a Macdonald Masambuka. Malinga ndi chikalatachi, a Muhosha aimitsidwa… ...
Ati za Chilima muiwale. Ngati aimile ndiye mwina chipani china basi koma kuja ku DPP, palibe amene akufuna a Mutharika achoke. Anthu ali nganganga pambuyo pa a Mutharika. Komiti yaikulu ya chipani cholamula cha DPP… ...
Top brass of Democratic Progressive Party (DPP) has endorsed President Peter Mutharika as torch bearer for the party in the 2019 polls, effectively breaking rank from Director of Youth Lewis Ngalande and former first lady… ...
Pamene moto umene anayatsa alamu a mtsogoleri wa dziko lino Mayi Callista Mutharika ukukhala ngati ukuvuta kuthimitsa, amene ali ndi udindo wa zothamangathamanga mu chipani cholamula a Ben Phiri ati kunena kuti Chilima atenge utsogoleri… ...
Ati iwo adanena kale kuti dziko liri mmanja mwa agalu koma ena adali kukayika, tsopano pano ndi uthenga umene afuula Mayi Callista Mutharika mu chipululu kuti a Peter azitaye ndiye kuti zaphelezera basi. Amene akutchulidwa… ...
After a week of breaking ranks with his brother-in-law who is also the President of the country and ruling DPP, former first lady Callista Mutharika was absent at a private memorial mass the Mutharika family… ...
Former First Lady Callista Mutharika has said Democratic Progressive Party (DPP) members will force Vice President Saulos Chilima to contest in the 2019 elections. Callista made the remarks in an interview with a local radio… ...
Wamisala anaona nkhondo. Ataopseza kuti ayenda buno bwamuswe pofuna kukakamiza boma la Malawi kuti lizinyonga anthu onse opezeka kuti apha albino, a Winiko akuoneka ngati tsopano atha kumvana Chichewa ndi Mtsogoleri wa dziko lino a… ...
A Kongeresi kodi mulipo apa? Musapite kutali chifukwa tili ndi uthenga wanu. Zija za Konveshoni mumadikila zija kuti ichitika lero pa 5, ku Mzuzu, ati muziiwale kaye. Mtsogoleri wa chipani chotsutsa cha MCP, a Lazarus… ...