Matani a chamba olemera makilogalamu oposa 1,150 omwe analandidwa kwa anthu osiyanasiyana chaka chino athilidwa moto ndi apolisi ku Mponela m'boma la Dowa dzulo. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Macpstson Msadala, apolisi atentha… ...
Articles By Ben Bongololo
Pamene dziko la Malawi likupitilira kukumana ndi mavuto osiyanasiyana pankhani yokhudza zachuma, katswiri pa nkhani ya zachuma a Betchani Tchereni wawuza a Malawi kuti ayembekezere kuti pali kuthekera koti mitengo ya zinthu pa msika ipitilira… ...
Apolisi m'boma la Mchinji ati matumba a simenti okwana 186 ndi omwe apezeka pakadali pano pa matumba okwana 600 kutsatira pomwe thilaki yomwe idanyamula matumbawa idayaka moto kwa Kholoni mbomali. Thilakiyi yomwe ndi ya kampani… ...
Mutale Mwanza yemwe ndi wachikondi wa oyimba odziwika bwino m'dziko lino, Tay Grin, wapulumuka pa ngozi yomwe inachitika dzulo pa 20 December ku Zambia. Nkhani yonse ikuti munthawi yomwe ngoziyi imachitika, a Mutale Mwanza amayendera… ...
Mkulu wina wa zaka 35 zakubadwa ku Lilongwe walamulidwa kukakhala ku ndende ndikukagwila ntchito ya kalavula gaga kwa zaka 21 kamba kopezeka olakwa pa mlandu wogwililira mwana wa zaka khumi. Malingana ndi mneneri wa apolisi… ...
Njonda zitatu zomwe zidanjatidwa pa mlandu okuba katundu zitavala ngati gulewamkulu kwa Chaima m'boma la Kasungu azipeza zolakwa pa mlandu wakuba ndipo azilamula kukagwira ntchito ya kalavula gaga kwa zaka 12. Nkhani yonse ikuti njondazi … ...
Apolisi m'dziko lino anjata a Shirieesh Betgiri yemwe ndi mkulu wapampando wakale wa kampani ya Salima Sugar kamba kokhudzidwa pa mlandu wakatangale wa ndalama zoposa K50 billion A Peter Kalaya omwe ndi mneneri wa apolisi… ...
Anthu atatu amwalira pamene anthu ena asanu ndi m'modzi avulala pa ngozi yomwe yachitika dzulo madzulo m'boma la Nkhotakota Yemwe ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Sub-Inspector Andrew Kamanga ati galimoto ya mtundu wa Sienta… ...
Nthambi yoona zanyengo ndi kusintha kwa nyengo m’dziko lino lachenjeza a Malawi maka akuchigawo chakum'mwera ponena kuti lero pa 14 December 2023, mvula yamphamvu ikhale ikugwa. Malingana ndi uthenga omwe watulutsa ndi mneneli wa nthambiyi,… ...
A Ken Msonda omwe ndi membala wa komitiyi yaikulu ya chipani cha DPP apepesa kwa mtsogoleri wa chipanichi a Peter Mutharika pa zomwe iwo akhala akuchita ndipo pano ati akufuna a Mutharika atengenso mpando wa… ...
Apolisi m'boma la Zomba amanga njonda ina kamba kopezeka ndi ma simukadi a lamya okwana 99 omwe njondayi imafuna kuti ilowetse mundende ya Zomba. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali, mkuluyi yemwe dzina lake ndi… ...
Kwa nthawi yoyamba tsopano kuchokera mchaka cha 2017, banki yayikulu pa dziko lonse ya World Bank yalengeza kuti ipeleka thandizo loti lithandizile mundondomeko yazachuma mdziko lino. Ndipo padakali pano yapereka ndalama zokwana 137 miliyoni dollars… ...
Zina ukamva kamba anga mwala, zina zikamachitika nkumati kodi ndiku Malawi komkuno? Inu anthu am'mudzi mwa Chimombo mdera la mfumu yayikulu Kachere m'boma la Dedza lero pa 12 December ali kukamwa yasa atapha njoka 301… ...
A Bon Kalindo akhala akusungidwabe mchitokosi cha apolisi uku akudikira chigamulo kuchokera kwa woweruza milandu a Muhammad Maxwell Chande lachisanu likudzali pa 15 December. A Kalindo anawanjata sabata latha m'boma la Zomba powaganizira kuti iwo… ...
A polisi mu mzinda wa Lilongwe ku Area 3, anjata a Jonathan Nkhosa yemwe ndi mphunzitsi wa kupulayimale wa zaka 51 zakubadwa, kamba kobera anthu powanamiza kuti ndi wapolisi. A Nkhosa akhala akuchita bodza kwa… ...