Malawi Police have burnt Chamba in Dowa
Matani a chamba olemera makilogalamu oposa 1,150 omwe analandidwa kwa anthu osiyanasiyana chaka chino athilidwa moto ndi apolisi ku Mponela m'boma la Dowa dzulo. Malingana ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Macpstson Msadala, apolisi atentha… ...
Anthu atatu amwalira pamene anthu ena asanu ndi m'modzi avulala pa ngozi yomwe yachitika dzulo madzulo m'boma la Nkhotakota Yemwe ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Sub-Inspector Andrew Kamanga ati galimoto ya mtundu wa Sienta… ...