A Malawi konzekani. Tsopano kukhala kupha makwacha kudzera pa tsamba la mchezo la Fesibuku komanso pa YouTube kuyambira chaka chomwe tichiyambe mawali cha 2024. Izi zili chomwechi malingana ndi zomwe wanena mkulu wa bungwe la… ...
Articles By Ben Bongololo
Mtsogoleri wadziko la Burundi Evariste Ndayishimiye yemwenso ndi mkatolika, wadzudzula mayiko a azungu kamba kolimbikitsa ma ufulu oti amuna kapena akazi azikwatirana okhaokha. Mkunena kwake wati izi ndizonyasa komanso zamalawulo kotero oterewa akapezeka aziyikidwa mbwalo… ...
Akayidi okwana 48 tsopano akhala akusimba lokoma kutsatira mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera wakhululukira ndikumasula akayidiwa mnyengo ino yachikondwerero cha khilisimasi komanso chaka chatsopano. Malingana ndi chikalata chomwe atulutsa a Oliver Kumbambe yemwe ndi… ...
Sukulu ya ukachenjede ya University of Livingstonia (Ekwenden Campus) yalengeza kuti yakweza sukulu fizi ndipo izi zikhudza ophunzira amene akudzayamba kumene komanso omwe omwe akupitiliza maphunzilo awo pasukuluyi. Malingana ndi chikalata chomwe sukuluyi yatulutsa, kusinthaku… ...
Apolisi ku Kasungu apempha anthu oyendetsa galimoto kuti ' 'asayiponde fadah' komanso asayendetse atapapira bibida komanso mankhwala ozunguza bongo pofuna kuti aliyense alowe mchaka chatsopano cha 2024 ndi moyo. Yemwe ndi komishonala wa apolisi mchigawo… ...
Pofika lero pa 27 December 2023, nyimbo ya Atoht Manje yomwe mutu wake ndi 'Nchape' tsopano yaoneledwa ka 1.1 miliyoni pa YouTube mu miyezi iwiri yokha. Iyi ndi nyimbo ya Atoht yomwe yaoneledwa kwambiri pa… ...
Reserve Bank of Malawi (RBM), yomwe ndi banki yayikulu m'dziko muno, yachenjeza kuti ithana ndi aliyense amene apezeke akukana ndalama ponena kuti inatha mphamvu ndipo potsindika za nkhaniyi a RBM ati ngakhale ma 1 tambala… ...
Zina ukamva ngati kumaloto ndithu. Apolisi m'boma la Kasungu amanga mfumu Mwimira yazaka 52 kamba kogwilira mdzukulu wake wazaka 16 ndikumpatsanso pathupi. Malingana ndi mneneri wa apolisi m'bomali a Joseph Kachikho, makolo amwanayu anadabwa kumuona mwanayu… ...
Apolisi ku Kasungu anjata bambo wina wazaka 29 wina yemwe akumuganizira kuti anapha mzake wazaka 28 dzana pa khilisimasi pomumenya ndi khasu m'mutu. Malingana ndi mneneri wa apolisi m'bomali a Joseph Kachikho ati bambo yemwe… ...
Maanja okwana 28 akusowa mtengo ogwira kamba ka mvula ya mphamvu yomwe yawononga nyumba komanso katundu osiyanasiyana kwa gulupu Mawawa, mfumu yayikulu Chulu m'boma la Kasungu. Mwakatundu wina wawonongeka kamba ka mvula ya mphamvuyi ndi… ...
Apolisi ku Kasungu amanga a James Phiri a zaka 36 zakubadwa kamba kopezeka akugulitsa zinthu zonga ngati feteleza zomwe anazipakira m'matumba a feteleza ndikumagulitsa ngati feteleza. Mkuluyu wamangidwa dzulo kutsatira anthu ena omwe anatsina khutu… ...
Black Nina yemwe ndi oyimba odziwika bwino m'dziko lino, anapita ku malo okwerera ndege ndi mpanda buleki (njinga) wake uku atanyamulirapo chibinyira cha zovala ndicholinga choti akweze njingayo mundege pawulendo wake waku jubeki. Malingana ndi… ...
Apolisi ku Ndirande tsopano akhala akusimba lokoma pamene nduna ya zachitetezo a Kenneth Zikhale Ng'oma lero yatsekulira nyumba zamakono zokwana 20 zomwe boma la a Lazarus Chakwera lamanga mgawo la nyumba 10,000 zomwe zikhale zikumangidwa… ...
Pulofeti wina kwa Jenda ali m’manja mwa apolisi kamba kogwililira mkazi wamwini yemwe anapita ku tchalitchi cha mneneriyu kuti akamupempherere pa vuto lakusowa mphatso ya mwana m'banja. Mayiyu yemwe wakhala miyezi itatu m'banja koma osatenga… ...
Pamene boma likukonzekera kulemba anthu ogwira ntchito mzipatala zaboma oposera 5,000, mkulu yemwe amayankhulapo pa nkhani za umoyo wayamikira boma la a Lazarus Chakwera kamba kochita chothekera poonetsa kuti anthuwa alembedwe ntchito. Vuto lakuchepa kwa… ...