Chilima apempha bata

Pamene anthu m’dziko muno akudikira mwachidwi chigamulo cha khothi pa mlandu wa za chisankho sabata lamawa, mtsogoleri wachipani cha UTM a Saulos Chilima apempha anthu onse kusunga bata. A Chilima amayankhula izi lachinayi kulikulu lachipanichi… ...