The Movement that is supposedly led by Malawi Vice President Saulos Chilima who has not yet communicated in person his political plans keeps gathering momentum. Now, musician Lucius Banda has joined the team. Days after… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
Zipani zotsutsa za Kongeresi ndi PP zinagwilizana zonyanyala mkumano okumana ndi a MEC pamene amafuna kumvana pa nkhani ya mmene kalembera wa anthu ovota akuyendela. Pa mkumanowu, nduna yofalitsa nkhani a Nicolas Dausi inapempha a… ...
The United Transformation Movement ( UTM) has gotten a huge boost ahead of the 2019 elections with top politicians announcing their joining of the movement. Speaker of Parliament, Richard Msowoya has joined the movement, reports… ...
Ati muziliyatsa la mtondo wadooka mukangomva za tambala wakuda. Ati pali Kongeresi, a Malawi nonse muzipita kukabisala ndithu osati kuthamangilako. A Nicolas Dausi amene ndi nduna yoona zofalitsa mauthenga komanso mneneri wa boma anauza msonkhano… ...
Ehede! Mwawakumbukila aja ankalandira za Lutepo aja uku akuzitukumula. Aja anali ndi galimoto kholophethe ali mu boma aja. Tsopano akuti maluzi awasasantha. Mneneri wa chipani cha PP a Noah Chimpeni wati chipanichi chilibe ndalama zoti… ...
Kukanakhala kuti pachiweru kunali mwambi, kaya a Chilima akanagwilitsa uti kaya? Koma pomaliza kulankhulapo pa mwambo odzodza ansembe a chikatolika pa Limbe Cathedral a Chilima anatsindika kuti kunalibe mwambi. Koma ngakhale panalibe mwambi ochoka kwa… ...
Akanakhala a Chilima ndi mikuluwiko yawo ija, mwina akanati n’konzen’konze ananyula maliro a eni; kapena akanangojama mulomowu ya Ma Blacks. Mkulu wa zipani zotsutsa boma mu nyumba ya malamulo amenenso ndi Mtsogoleri wa chipani chotsutsa… ...
Ikuvuta kuijama iyiyi. Akanakhala a Chilima mwina akanatimasula kuti paja akakhala pa mkhate si umo avutila kupha. A Malawi ochuluka ati Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika atule pansi udindo wawo ndipo afufuzidwe. Pa… ...
Akanakhala a Saulos Chilima kuti akuthilira ndemanga pa nkhaniyi mwina akanati andione andione anakhalira zinthu zake zomwe; kapena akanati n’konze n’konze ananyula a weni maliro? Aphungu amene ali patsogolo poyendetsa ntchito ya a Chilima kuti… ...
Zikamatha zisankho za 2019, a mabungwe akufuna achinyamata azakhale adzadza mu ma udindo ovoteledwa. Koma malinga ndi amabungwe amene asonkhana pamodzi kuti aonetsetse kuti achinyamata agwetsa madala mu zisankho, bungwe loona za zisankho la MEC… ...
National Coordinator for Chilima Movement Noel Masangwi has claimed that Malawi President Peter Mutharika is controlled by First Lady Gertrude Mutharika. According to Zodiak, Masangwi told a rally in Blantyre that Mutharika follows the decisions… ...
He has instincts for creating hit songs out of existing music hits, a description that perfectly fits Malawi's award winning urban artist Martse. The Lilongwe based artist recently unleashed a 'remake' or sampling of a… ...
Zida zija anasula a Mutharika kuti anyenye a Chilima ndi owatsatila tsopano zilibe ntchito. Kutukwana konse amachita Mayi Kaliati nako kulibe fungo. Tsogolo silikuoneka bwinobwino. A Chilima ati afotokoza bwino lino. Atakola chidwi cha a… ...
Inu owelenga Baibulo, mwaikumbukila nkhani ya bulu anakwelapo Yesu ija akukalowa mu Yerusalemu? Ngati mwayiwala, dikilani tikukumbutseni. Paja Yesu anatuma ophunzila kuti apite mmudzi, ndipo akapezamo bulu ndipo akamumasule ndi kumupititsa kwa iye. Aliyense akafunsa,… ...
The writing might just be on the wall for Malawi's Afro Pop singer Dan Lu on his marriage to Emmie Kamkweche, Malawi24 has been told. A source close to the two has told Malawi24 that… ...