Dausi
Chipasupasu chija chafika. Wina kwake, winanso uko. Wadya balalikani akuchitika ku chipani cholamula cha DPP. Mneneri wa boma a Nicholas Dausi adzudzula kolimba wachiwiri kwa Mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima kamba konena kuti… ...
Saulos Chilima, Peter Mutharika
...DPP Govt. is so corrupt The centre in the ruling Democratic Progressive Party (DPP) is no longer holding. For those party diehards who thought vice-president Saulos Chilima can be called back to order, they should… ...
Peter Mutharika
A Chilima ndi anthu ena onse amene akunena kuti a Mutharika apume ndi anthu a bizinesi ndipo akufuna kugulitsa chipani, atelo a Mutharika. Pa mwambo otsegulila trade fair mu mzinda wa Blantyre, a Mutharika anasintha… ...
Malawi elections MEC
For the first time since Malawi adopted multiparty democracy, government will fund the general elections without donor support. Minister of Finance Goodall Gondwe revealed this when presenting the K1.5 trillion 2018/19 national budget in Lilongwe… ...
George Chaponda
Anthu amene safunila a George Chaponda zabwino, anthu amene asanadye pemphero lawo limakhala lopempha Mulungu kuti mwina angozimitsa a Chaponda, ati ndi amene ankapanga upo ofuna kugwetsa a Chaponda koma alephera. Nduna yakale ya zaulimi… ...
Bushiri
Ati asiya zokokanakokana. Tsopano ndi amodzi ndipo agwilila ntchito limodzi. Ndipo apo mwaona Bushiri, yembekezani kuona Mboro. Mneneri Shepherd Bushiri amene ali ku South Africa ati wagwilizana ndi M’busa wa ku South Africa komweko wa… ...
Lazarus Chakwera
Inu a DPP, zichedwani ndi kulumana. Anzanu a Kongeresi ndiye zawo zayela anga achapa ndi Boom. Zija zomati a Kaliwo, a Msowoya ndi a Kabwila akatenga chiletso kapena apilikitsidwa mu chipani, ndi nkhani yakale tsopano.… ...
Prophet Shepherd Bushiri
M’busa amene amaziti ndi mneneri Shepherd Bushiri analowa mchitolokosi cha a Polisi m’dziko la South Africa usiku wa loweruka. Bushiri amene akufufuzidwa pa mlandu okuba ndalama ku South Africa kuti azizabisa ku Malawi kuno, anaitanidwa… ...
Enoch Chihana
Alliance for Democracy (Aford) President Enoch Chihana has taken an injunction restraining other party members from holding a convention on Sunday. There are wrangles in the party over the date of the convention with a… ...