Chipasupasu chija chafika. Wina kwake, winanso uko. Wadya balalikani akuchitika ku chipani cholamula cha DPP. Mneneri wa boma a Nicholas Dausi adzudzula kolimba wachiwiri kwa Mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima kamba konena kuti… ...
Articles By Kondwani Mkhalipi-Manyungwa
...DPP Govt. is so corrupt The centre in the ruling Democratic Progressive Party (DPP) is no longer holding. For those party diehards who thought vice-president Saulos Chilima can be called back to order, they should… ...
A Chilima ndi anthu ena onse amene akunena kuti a Mutharika apume ndi anthu a bizinesi ndipo akufuna kugulitsa chipani, atelo a Mutharika. Pa mwambo otsegulila trade fair mu mzinda wa Blantyre, a Mutharika anasintha… ...
Sizili bwinotu a President ndipo ena amene akumabwela pamaso panu ndi kumati ndi anu, musawamvele chifukwa usiku akumanka nakanyonyomala kwa wachiwiri wanu kukachongetsa. A Lewis Ngalande amene ndi mkulu wa achinyamata muchipani cholamula cha DPP… ...
For the first time since Malawi adopted multiparty democracy, government will fund the general elections without donor support. Minister of Finance Goodall Gondwe revealed this when presenting the K1.5 trillion 2018/19 national budget in Lilongwe… ...
Ndi lerotu neba pa Balaka. Kukakhala ku banja la maule, usikuwu anagona tulo tofa nato podziwa kuti malo awo mu ma semi alipo kale. Palibe olanda. Nyerere kapena kuti manoma ali ndi ntchito yaikulu lero… ...
Anthu amene safunila a George Chaponda zabwino, anthu amene asanadye pemphero lawo limakhala lopempha Mulungu kuti mwina angozimitsa a Chaponda, ati ndi amene ankapanga upo ofuna kugwetsa a Chaponda koma alephera. Nduna yakale ya zaulimi… ...
Ati asiya zokokanakokana. Tsopano ndi amodzi ndipo agwilila ntchito limodzi. Ndipo apo mwaona Bushiri, yembekezani kuona Mboro. Mneneri Shepherd Bushiri amene ali ku South Africa ati wagwilizana ndi M’busa wa ku South Africa komweko wa… ...
Nkhondo ija ya Absalom ndi Davite yavuta ku chipani cholamula cha DPP. Ndipo pamene aliyense akukokela mbali yake, nawo ana a mu sukulu za ukachenjede ati asatsalire. Ana a mu sukulu za ukachenjede a chipani… ...
Inu a DPP, zichedwani ndi kulumana. Anzanu a Kongeresi ndiye zawo zayela anga achapa ndi Boom. Zija zomati a Kaliwo, a Msowoya ndi a Kabwila akatenga chiletso kapena apilikitsidwa mu chipani, ndi nkhani yakale tsopano.… ...
Munali phwete mu nyumba ya malamulo pamene wachiwiri kwa Mtsogoleri wa chipani cha PP anaima mu nyumbayo. A Kamlepo Kalua amene amayankha pa zimene Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika anayankhula potsegulila nyumbayi anapempha… ...
Inu owelenga Baibulo, olitsata bwino, mwaidziwa nkhani ya uja Abisalomu anafuna kulanda ufumu wa Bambo ache kenako ndikufa ngati galu? A Nkasa ati Abisalomu uja, mu masiku a lero, ndi wachiwiri kwa a Peter Mutharika,… ...
M’busa amene amaziti ndi mneneri Shepherd Bushiri analowa mchitolokosi cha a Polisi m’dziko la South Africa usiku wa loweruka. Bushiri amene akufufuzidwa pa mlandu okuba ndalama ku South Africa kuti azizabisa ku Malawi kuno, anaitanidwa… ...
Alliance for Democracy (Aford) President Enoch Chihana has taken an injunction restraining other party members from holding a convention on Sunday. There are wrangles in the party over the date of the convention with a… ...
President Peter Mutharika has declared that he is not voluntarily quitting to pave way for his younger Vice President Saulos Chilima. Speaking upon his return from the United Kingdom, Mutharika said that he will be… ...