Ubwenzi wa Tay Grin ndi Mutale Mwanza ukuoneka uli pendapenda potsatira uthenga omwe mkaziyu walemba pa tsamba lake la mchezo. Uthengawu ukusonyeza kuti mkaziyu wasweka mtima ndi zomwe bwenzi lake la muchita ngakhale zifukwa zake… ...
Articles By Peter Mavuto
Kazembe wa dziko la Amerika m'dziko muno, David Young, watsanzika potsatira kutha kwa nthawi yake ya ukazembe. Mu chikalata chomwe ofesi ya ukazembe wa dziko la Ameleka yatulutsa chati a David akhala pa udindo wa… ...
Bungwe la Evangelical Association of Malawi (EAM) lapempha anthu onse dziko muno kuti pakhale mapemphero apaderadera opemphelera mvula kamba ka ng'amba yomwe yakhudza m'dera ambiri m'dziko muno. Chikalata chomwe wasainira ndi mlembi wamkulu m'bungweli, M'busa… ...
Apolisi m'boma la Nkhotakota amanga mkulu wa za malonda ku Chidewe ADMARC, Patrick Duston wa zaka 35, pomuganizira kuti ndi amene anazembetsa matumba 124 achimanga a ndalama zomwana 7.3 miliyoni. Mneneri wa apolisi ya Nkhunga,… ...
Apolisi m'boma la Chiradzulu akusakasaka anthu omwe apha mai wa zaka 78 zakubadwa, Edina Makhumba. Mbandazi zathawaso ndi foni ya manja tamabatani, Nkhuku folo, zofunda, ufa wachimanga olemera 5 kilogalamu komaso ndalama yokwana K20,000. Mneneri… ...
Akulu akulu a boma la Machinga ati mitengo yomwe inali pa malo okwana mahekitala okwana 50 mu nkhalango zosiyasiyana yadulidwa mu zaka wiri zapitazo. Wapampando mu khosolo ya Machinga, Cydreck Stande, anati mchitidwewu ukupitilila kamba… ...
Namondwe wa Freddy komanso mchitidwe okuba zichitsulo cha njanji ndi zina mwa zomwe zachedwetsa ntchito yokonzaso njanji ya makilomita 72 ya Limbe-Sandama. Nduna yoyang'anira mayendwe komaso ntchito, Jocobo Hara, wati pakadali pano sizikudziwika nthawi yeniyeni… ...
Akatswiri pa nkhani zolosela nyengo m’dziko muno ati a Malawi ayembekezere kulandila mvula yochepa mwezi uno wa February moyerekeza ndi mwezi watha. Izi zanenedwa kudzera mu ulosi umene nthambi yoona za nyengo yatulutsa okhudza kagwede… ...
Unduna wa za maphunziro mogwirizana ndi bungwe la Malawi Communication Regulatory Authority (MACRA) wakhazikitsa gawo lachiwiri la maphunziro kwa anthu amene amaphunzitsa chiyankhulo cha manja kwa anthu amene ali ndi ulumali . Maphunzirowa amene akuchitikira… ...
Apolisi m'boma la thyolo akusaka bambo Nyozani Phiri a zaka makumi atatu zakubadwa powaganizira kuti ndi amene apha mkazi wawo wachinayi, Lucy San wa zaka makumi atatu zakubadwa. Wachiwiri kwa mneneri wa apolisi m'boma la… ...
Dziko la Israel lati likufuna a Malawi okwana 100,000 kuti akagwire ntchito zosiyanasiyana ku Israel. Izi zayankhulidwa lero pamene nduna ya zachuma mu dziko la Israel, Nir Barakt, anali ndi mkumano ndi mlembi wamkulu mu… ...
Wapampando wa bhodi ya Mulhako wa Alhomwe watsutsa mphekesera yoti bhodiyi yachotsa mtsogoleri wakale wa dziko lino a Peter Mutharika ngati woyang'anira bungweli. Mukuyankhula kwawo pa msonkhano wa atolankhani mu mzinda wa Blantyre lachiwiri, Muchanakwaye… ...
Nthambi yoona za nyengo yati madera ambiri m'dziko muno maka mu chigawo cha kum'mwera ndi pakati, ng'amba ikhala ikupitilira kwa sabata imodzi kamba koti mphepo ya mvula ikuombera dziko la Tanzania. Ngakhale izi chili chomwechi, mkulu… ...
Due to the continued spread of cholera, authorities in Zambia say schools in the country will remain closed until February 12, 2024 to protect the lives of people. Education minister Douglas Syakalima said at a… ...
Mkulu wa Mwanza Social Welfare, a Mary Msidwa, ati boma la Mwanza lakwanitsa kuthetsa maukwati a ana achichepere okwana 118 mu chaka cha 2023. A Msindwa anena izizi lero pamene anali ndi zokambilana ndi khosolo… ...