Unduna woona mphamvu za magetsi m'dziko muno wati boma likufuna kuti pofika chaka cha 2030, anthu 50 pa anthu 100 aliwonse adzakhale akugwiritsa ntchito magetsi. Pakali pano anthu 27 pa anthu 100 aliwonse ndi amene… ...
Articles By Peter Mavuto
Nthambi ya apolisi dziko muno yachotsa ntchito apolisi awiri amene amagwira ntchito m'boma la Thyolo chifukwa cha kulephera kusunga mwambo komaso kujomba ku ntchito mopanda chilolezo. Mu kalata yomwe wasainira ndi wachiwiri kwa mkulu wayang'anira… ...
Bungwe la Malawi Red Cross Society lati lidzipereka kuthandiza anthu omwe akhudzidwa ndi kusefukira kwa madzi mu chigawo chapakati ndi kumpoto kwa dziko lino chifukwa ndipo lati chiwerengero cha anthu omwe akusowekera thandizo ndi malo… ...
Mtsogoleri wa chipani cha Mzika Coalition, Milward Tobias, wapempha a Malawi kuti asatope pofuna kuthana ndi mavuto a zachuma omwe ali mu dziko muno. Izi zayankhulidwa pamene dziko lino likukumbukira amatiliti amene anamenyera ufulu kuti… ...
Asilikali a dziko lino atenga nawo gawo populumutsa anthu pafupipafupi 200 omwe akhudzidwa ndi madzi osefukira ku Dwangwa m'boma la Nkhotakota. Malingana ndi lipoti lochokera ku khonsolo la Nkhotakota, asilikaliwa akugwiritsa ntchito mabwato awo apa… ...
Mtsogoleri wakale wa dziko lino, a Joyce Banda, apempha boma ndi mabungwe omwe akugawa chimanga kwa anthu omwe akhudzidwa ndi njala m'dziko muno kuti achite machawi kufikira madera ambiri anthu ambiri akhudzidwa ndi mavuto osowa… ...
Mneneri Shepherd Bushiri kudzera pansi pa bungwe la Shepherd Bushiri Foundation (SBF) wasainirana mgwirizano ndi katakwe pa nkhani yochita ma filimu wa m'dziko la Nigeria, Nkem Owoh, lamulungu lapitali mu mzinda wa Lilongwe ngati njira… ...
Mtsogoleri otsutsa boma mu nyumba ya malamulo yemwenso ndi mkulu wa amai mu chipani cha DPP, Mai Mary Navicha, wati amai ambiri apangidwa chipongwe powagwirira pa chipolowe chomwe chinali dzulo mu mzinda wa Lilongwe. Dzulo… ...
Boma kudzera ku ndondomeko ya za chuma cha dziko lino ya chaka cha 2024/2025 laika ndalama zoyambilaso ntchito yomanga bwalo la zamasewero a matimu a FCB Nyasa Big Bullets komanso Mighty Mukuru wanderers. Ntchitoyi inaima… ...
Katswiri pa kapezedwe ka chakudya dziko wati ndondomeko ya chuma ya chaka cha 2024/25 ikuyenela kuthandizira ulimi wa mthilila m'dziko muno pofuna kuthana ndi mavuto omwe adza kamba ka ng'amba yomwe yakhudza dziko lino. Ronald… ...
Bwalo la majesitireti m'boma la Mangochi lagamula Martha Victor a zaka 32 zakubadwa kukhala ku ndende kwa zaka zitatu chifukwa chovulaza mwa omupeza kamba koti anakodzera nyumba. Malinga ndi mboni ya boma, Ted Namaona wati… ...
Kampani yopanga shuga m'dziko muno ya Illovo yalengeza kuti ili ndi masomphenya okonza mphamvu za magetsi payokha kuti ichepetse ndalama zimene kampaniyi imaluza kulipira magetsi ku ESCOM. Mkulu wa kampaniyi, Lekani Katandula, ndiye anayankhula izi… ...
Banki ya NBS yalonjeza kuthandiza anthu amene akhudzidwa ndi njala dziko muno. Mkulu wa nthambi ya bankiyi ku Limbe, Twaibu M’nani, anayankhula izi dzulo pa 18 February, 2024, m'boma ya Chiradzulu kumene bankiyi imagawa ufa… ...
Bungwe la Southern Region Water Board (SRWB) yati ili ndi chikonzero chomanga dam lalikulu ku Domasi m'boma la Zomba limene lithandizire kuonjezera madzi amene bhodiyi imagawa komanso kuthandizira pa ulimi wa mthilira, ulimi wa nsomba… ...
Pamene maiko ochuluka amakumbukira tsiku la nyama ya Ngaka (pangolin) dzulo pa 17 February, akuluakulu oyang'anira nkhalango yotetezedwa ya Liwonde m'boma la Machinga ati mchitidwe ogwira ndi kuzembetsa nyamayi wachepa ku nkhalangoyi. Mkulu oyang'anira nkhalangoyi… ...