...50+1 ndiyomwe igwiritsidwe ntchito.... Bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lapempha anthu kuti akhale odekha komanso asunge bata ndi mtendere pomwe dziko lino likhale likuchita chisankho cha mtsogoleri wadziko lachiwiri lino.… ...
Bungwe loyendetsa zisankho m'dziko muno la MEC lapempha anthu omwe analembetsa pa mavoti kuti akatsimikize ngati maina awo ali mu nkaundula ndipo izi zichitika lachitatu ndi lachinayi sabata ino. Watsimikiza zankhaniyi ndi mneneri wa bungwe… ...