M'modzi mwa akuluakulu a mgwirizano wa Tonse, a Patricia Kaliati, ayamikira wapampando wa bungwe loyendetsa zisankho la MEC a Justice Dr Chifundo Kachale ponena kuti akugwira bwino ntchito. A Kaliati amayankhula izi mu mchipinda cha… ...
Articles By Archangel Nzangaya
...50+1 ndiyomwe igwiritsidwe ntchito.... Bungwe loyendetsa zisankho m’dziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lapempha anthu kuti akhale odekha komanso asunge bata ndi mtendere pomwe dziko lino likhale likuchita chisankho cha mtsogoleri wadziko lachiwiri lino.… ...
Chiwelengero cha anthu omwe apezeka ndikachilombo ka Corona komwe kakumayambitsa matenda a COVID-19 chafika pa anthu 481 tsopano. Watsimikiza za nkhaniyi ndi Dr John Phuka omwe ndi wapampando wagulu lomwe mtsogoleri wadziko lino a Peter… ...
After a couple of months without live sporting events due to the COVID-19 pandemic, DStv and GOtv customers who are sport fanatics can finally breath a sigh of relief following the return of the live… ...
Bungwe loyendetsa zisankho m'dziko muno la MEC lapempha anthu omwe analembetsa pa mavoti kuti akatsimikize ngati maina awo ali mu nkaundula ndipo izi zichitika lachitatu ndi lachinayi sabata ino. Watsimikiza zankhaniyi ndi mneneri wa bungwe… ...
A political analyst has faulted President, Peter Mutharika for re-appointing Dr Jean Mathanga and Linda Kunje as commissioners of the Malawi Electoral Commission (MEC). On Sunday evening, the office of the president and cabinet announced… ...
A video director in the country says Malawi is making strides in music video shooting, editing and quality. In an interview with this publication VJ Ken who was born Kenneth Makina said in the past… ...
The High Court in Mzuzu has found three people with a murder case to answer over the killing of a Nkhatabay man with albinism. On December 31 in 2018, Yassin Kwenda Phiri, 54, was brutally… ...
Africa's leading entertainment providing firm, MultiChoice has launched DStv and GOtv Self-Service Apps. Confirming the development was Managing Director at MultiChoice Malawi Gus Banda who said with this newly launched app, DStv and GOtv customers… ...
Five buses carrying 285 Malawian nationals coming from South Africa have arrived in the country through the Mwanza formation. This is a Malawi government program to repatriate citizens who were stranded in South Africa due… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika adzudzula mchitidwe wa zipolowe pandale omwe wakula m’dziko muno koma ati gwero lazonsezi ndi ndikuyankhula udyo kwa atsogoleri azipani zotsutsa. A Mutharika amayankhula izi lachisanu kudzera kwa owayankhulira… ...
Bungwe la eni maminibasi m'dziko muno la Minibus Owners Association of Malawi (MOAM) lati oyendetsa ma minibasi onse omwe sanatsitsebe mitengo yawo akuyenera kumangidwa. Wayankhula izi mlembi wamkulu wa bungweli a Felix Mbonekera omwe anati… ...
An association for independent school owners, the Independent Schools Association of Malawi (ISAMA), has threatened that it will call for demonstrations if government fails to open schools by 1st June this year. This is according… ...
Anthu asanu ndi atatu (8) omwe anapezeka ndikachilombo ka corona komwe kakumayambitsa matenda a COVID-19, athawa pamalo omwe amawasungira kwa Kameza mu nzinda wa Blantyre. Watsimikiza zankhaniyi ndi nkulu wa zaumoyo mu mzindawu Dr Gift… ...
Ku Malawi, chiwelengero cha anthu omwe apezeka ndi kachilombo ka Corona komwe kakumayambitsa matenda a Covid-19 chafika pa anthu 101 tsopano. Watsimikiza za nkhaniyi ndi nduna ya zaumoyo m'dziko muno a Jappie Mhango omwe amayankhula… ...