Lero komiti yosungitsa mwambo ku chipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive (DPP) yakumana ndi a Kondwani Nankhumwa, Mark Botoman komaso a Cecilia Chazama koma osewa sakuulura momwe zathera, pamene a Grezelder Jeffrey sanafike kumaloku. Anayiwa… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Following the Supreme Court of Appeal ruling on application by the former Vice President (South) for the Democratic Progressive Party (DPP) Kondwani Nankhumwa, former Secretary General Grezelder Jeffrey and former Director of Women Cecelia Chazama,… ...
Malawi Women's National Football Team forward Temwa Chawinga who was recently named world’s top goal scorer of the year 2023, has joined Kansas City Current Women's Team in the United States of America. The prolific… ...
Patangodutsa maola ochepa khothi la apilo ku Blantyre litakana pempho la a Kondwani Nankhumwa, Grezelder Jeffrey komaso Cecilia Chazama loti abwezeletsedwe mmaudindo awo ku chipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive (DPP), a Nankhumwa ati achilandira… ...
Yalimba nkandilo! Pomwe a Kondwani Nankhumwa, a Grezelder Jeffrey komanso a Cecilia Chazama amafuna bwalo la apilo liwabwezeretse pa maudindo awo mu chipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive (DPP) komaso kuwapatsa chiletso kuti asakaonekere ku… ...
Inde chakachi achilowa nawo komatu achilowa nkhope zawo zitatupa fufufuu ngati mandazi. Wilson Masamba komanso Limbani Lano omwe kwathu kuno timawati anamatetule azigogodo, awona chidameta nkhanga mpala ku Tanzania komwe agwebedwa ngati mawa kulibe mpaka… ...
Pomwe zafika pano, yemwe sanaonelebe kanema othyakulidwa kwathu konkuno wa ‘School Days', akutengedwa otsalira zedi m'makwalalamu. Kanema uyu wazula mitima ya a Malawi ochuluka ndipo omwe anaphunzira sukulu zogonera konko akumangomwetulira akamaonera kwinaku akuwasimbira ana… ...
A Kondwani Nankhumwa, a Grezelder Jeffrey komanso a Cecilia Chazama ati sakumvetsetsa kuti bwalo la milandu ku Lilongwe linavomeleza kusinthidwa maudindo awo mu chipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive (DPP) ndipo atatuwa akagwadwa ku bwalo… ...
The man behind the translation of English versions of movies into the local language, Chichewa Clyton Thomas also known as Akila, has won best actor of the year and the entertainer of entertainers at the… ...
The Mangochi Senior Resident Magistrate Court sentenced 40-year-old Prophet and founder of Supernatural Embassy Ministry, Christopher Phiri, to 19 years in jail for having sexual activity with his 16-year-old biological daughter whom he accused of… ...
Mneneri Christopher Phiri wa zaka 40 yemwe ndi mwini utumiki wa Supernatural Embassy ku Mangochi, wagamulidwa kukaseweza jere zaka khumi, mphambu zisanu ndi zinayi (19) kamba koseweretsa malo obisika a mwana wawo wa mkazi wa… ...
Pomwe pali kusamvana pa nkhani yamalipiro pakati pa achinyamata omwe akugwira ntchito mdziko la Israel ndi ma agent omwe adawatumiza mdzikolo, boma kudzera mwa Kazembe woimila Malawi ku Israel lati achinyamata omwe sakufuna kuti ndalama… ...
Mayi yemwe amagwira ntchito yosamala maluwa a Tiyanjane Mlangeni, omwe akuganizilidwa kuti ndiosasunga pakamwa ndipo akhala akuwulura zinsinsi zochuluka zokhudza kumpanda, inde ku nyumba ya boma, achotsedwa ntchito. Izi ndi malingana ndi kalata yomwe boma… ...
Kampani ya mafoni a m’manja ya Airtel Malawi yati kuyambira sabata ya mawa itsitsa ndi 1 kwacha mitengo yomwe makasitomala ake amalipira akamayimbira lamya kapena kutumiza mauthenga ku ma netiweki ena. Izi ndi malingana ndi… ...
The High Court in Lilongwe says Democratic Progressive Party (DPP) president Peter Mutharika’s decision to shift Grezelder Jeffrey Kondwani Nankhumwa, and Cecilia Chazama to other positions in the party did not violate the political rights… ...