Mayi yemwe amagwira ntchito yosamala maluwa a Tiyanjane Mlangeni, omwe akuganizilidwa kuti ndiosasunga pakamwa ndipo akhala akuwulura zinsinsi zochuluka zokhudza kumpanda, inde ku nyumba ya boma, achotsedwa ntchito. Izi ndi malingana ndi kalata yomwe boma… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Kampani ya mafoni a m’manja ya Airtel Malawi yati kuyambira sabata ya mawa itsitsa ndi 1 kwacha mitengo yomwe makasitomala ake amalipira akamayimbira lamya kapena kutumiza mauthenga ku ma netiweki ena. Izi ndi malingana ndi… ...
The High Court in Lilongwe says Democratic Progressive Party (DPP) president Peter Mutharika’s decision to shift Grezelder Jeffrey Kondwani Nankhumwa, and Cecilia Chazama to other positions in the party did not violate the political rights… ...
Mpira wamapazi ku Malawi: Timu yaing'ono ya Mighty Mukuru Wanderers yomwe makolo ake atuluka chakachi opanda chikho, imayenera kumenya ma “finals” awiri, ina ku Dowa ndi ina ku Machinga, Lamulungu likubwerali. Timu ya Wanderers Reserve… ...
Apolisi mdziko muno ati anthu asanu ndi atatu amwalira kamba ka ngozi za pa msewu pa tsiku la khilisimisi chaka chino. Wanena izi ndi wachiwiri kwa ofalitsa nkhani za apolisi m’dziko muno a Alfred Chimthere… ...
Unduna owona za chilengedwe ndi kusintha kwa nyengo, mogwirizana ndi nthambi yowana za zanyengo, wati pali chiopsyezo choti sabata ino madera ena m'dziko muno makamaka mchigawo cha kum'mwera kukhala madzi osefukira. Izi ndi malingana ndi… ...
Mtsikana wa wazaka 16 m’boma la Mzimba wadzipha podzimangilira mu mtengo pafupi ndi nyumba yakwawo kamba koti mayi ake anamukalipira chifukwa chomwa mowa mwauchidakwa tsiku la khilisimisi. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa polisi ku Jenda… ...
Arava Farm yomwe ndi imodzi mwa kampani zomwe zatenga a Malawi kukagwira ntchito mdziko la Israel, yati anthu mdziko muno asadere nkhawa za umoyo wa azibale awowa ponena kuti anthuwa akugwira ntchito mosangala kwambiri, ndipo… ...
After decades of long journeys to fetch water from unsafe sources, people in Chiradzulu district can now afford a great sigh of relief as they now have access to clean and safe water through mechanized… ...
“Osewera tagwirizana kutenga zikho zonse,” mhuuu! Anakadziwa sanakayankhula, maloto a chumba enieni, chimanjamanja ikutuluka m'chakachi. Tsoka la mfutso lopita pa moto kawiri ndipo kupsa kwake ndi kwa chigumu, pansi ndi pa mwamba. Mukutipheranji? Walira movetsa… ...
Amid increased cases of unsafe abortion amongst girls and women in Malawi, a non-governmental organization, Nyale Institute, has encouraged authorities and relevant stakeholders to review the country’s sexual reproductive laws. This is according to Nyale… ...
Bungwe la Roads Fund Administration (RFA) lawopseza kuti oyendetsa galimoto omwe agwidwe akudutsa mokakamiza pa ma “tollgate” osalipira ndalama, alipira chindapusa cha ndalama yokwana 1 miliyoni kwacha. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe bungwe la… ...
Mtsikana wazaka 20 yemwe anamangidwa mu 2021 kamba kakupha “mwangozi” mwana wake wa chaka chimodzi ndi miyezi 9, lero ali ndi chimwemwe chodzadza tsaya pomwe wamasulidwa ndipo wauzidwa kuti asapalamuleso mlandu uli onse kwa chaka… ...
The University of Malawi Workers Trade Union (UWTU) has demanded clarification from the university's Registrar on why the Daily Subsistence Allowance (DSA) for workers in top grades has unjustifiably been increased more than the allowance… ...
Ma bishopu a mpingo wa Katolika pansi pa bungwe la Episcopal Conference of Malawi (ECM), ati zomwe alamula kuti a nsembe asamapeleke mdalitso uli onse kwa anthu okwatilana amuna kapena akazi okhaokha, sizikutanthauza kuti iwo… ...