Image: Unsplash The world of esports has grown significantly in Kenya over the past few years, and one of the most popular titles within this space is Starcraft. With more bookmakers offering betting options on… ...
Articles By Lindiwe Sambalikagwa
In a shocking turn of events, the Electricity Supply Corporation of Malawi (ESCOM) has terminated an employee's contract over a 2020 Facebook post criticizing the Chakwera administration's failure to end loadshedding. The termination is seen… ...
Mwayidziwa bwino nyimbo ya mwana ndi mwana imene amakonda kuimba ma Palestina? Kukhala ngati mwana wake amanena achabale awo a Mighty Mukuru Wanderers kapena kuti Manoma. Zawaonekera lero atalepherana ndi timu ya Mighty Tigers. Atayamba… ...
Police in Salima have arrested a 67-year old woman for allegedly raping a 12- year-old boy and infecting him with Sexually Transmitted Infections. According to Spokesperson for Salima Police Station Jacob Khembo, the suspect has… ...
…150 miliyoni ya anthu inasokonekera…musamvere zachambazo - akutero Kachamba Ngwira Inu amene mumaziona mutatsegula kampani zanu za sopo, kaya kupanga shuga, enanu ma juwisi ndi zimzake, iwalani zimenezo. Mkulu analonjeza zokhutitsa a Malawi ndi luso… ...
…apolisi awayendere — katswiri wa chitetezo Ena akukanika kuyankhula momasuka chifukwa akuopa kukupidwa makofi. Ena ndiye angomasula. Koma a Malawi ochuluka aoneka odabwa ndi vidiyo imene watulutsa phona wa mu mzinda wa Blantyre, Ichocho, yolengeza… ...
Oyimba wa kale wa chamba cha hip hop Jolly Bro (JB) akupitirizabe kuthira makala a Malawi a ku South Bend ku Amereka. Pano waonjezera mkwiyo kwa mkulu wa dambwe Tay Grin. Ati kumene akukayimba kumeneko… ...
…52 miliyoni yanga ya bet yapita Zija ankapanga azimalume kalekale zomakunyengelera chimanga chophika kuti akonze nsewu zamuonekera James Chaola amene anawina bet ya 52 miliyoni. Kusiyana kwake ndi koti iye sanamubwenzere ndi komwe chenje, amuuza… ...
…akushopa pa kaunjika wa kumeneko Kumudzi kuno Lulu ndi namandwa oyimba. Zithunzi zake za makabudula pamene ali ku Amereka zikuoneka za mtengo wa patali. Koma oyimba Jolly Bro kapena kuti JB ati tisatengeke nazo. Ku… ...
Tanzanian combat engineers have left Malawi about two weeks after they were deployed to restore and rehabilitate infrastructure destroyed by Cyclone Freddy. The 59 were sent to the southern region of the country towards the… ...
…Wadzudzula mchitidwe ozithandiza wekha Kudya beti ndi kosangalatsa inde. Kwa ena kupambana mayeso kumene kutha kukhala chinthu cha mtengo wa pamwamba. Koma zonsezi sizingafike pa kugonana. Kugonana ndicho chinthu chokongola kwambiri pa dziko pano, watero… ...
…boma likupanga malamulo atsopano okhaulitsa ma dalaiva a chakumwa Phungu wa dera la pakati mu boma la Mwanza a Nicolas Dausi anachemetsa ku nyumba ya malamulo pamene anadzudzula nduna ya boma kuti imanyogodola anthu omwa… ...
…misonkho ikuthera ma lendi mu Lilongwe…nduna ndi ya nsanje yotenga mkazi ngati kapolo…ana 5, amayi 5 Nkhani ya nduna yoona za masiketi, imene pena imapanganso za chuma, ikupitilira. Mayi amene anabwera kugulu ndi kulengeza kuti… ...
Zoti tiri pa chisoni sizinaoneke. Zoti tate wathu ndi m'busa sizinaonekenso. Pena kumati mwina malaya ofiyira tinavala lero anamusokoneza mmaso Mo Salah kuti amayesa ndi Manchester United. Chifukwa atiswa ndipo atisambitsa chokweza. Olo naye kochi… ...
Chithyola More Malawians working at Mwanza Border will lose their jobs when the One-Stop Border post is launched, government has revealed. The losses are a direct opposite that President Lazarus Chakwera promised during his presidential… ...