Part of the M5 Road has been washed away at Phakwe, 54 kilometres from Kaphantenga, and motorists have been advised to use the Nkhotakota-Kasungu Road. Roads Authority (RA) spokesperson Portia Kajanga says the road has… ...
Articles By Lindiwe Sambalikagwa
Malawi Judiciary employees have started a strike today to force government to approve a review of their conditions of service. Among others, the workers want their allowances and monthly salaries to be raised. Judiciary Union… ...
A trove of Twitter Files released this week has revealed that Twitter bosses and senior employees read people's DM (Direct Messages). Twitter Files are serialised in two parts. The files were leaked and published by… ...
Pamene dziko linatangwa ndi kumangidwa kwa Mayi Chizuma, bwalo ku Lilongwe linatangwa ndi kuzenga milandu Mayi Dorothy Shonga komanso mkulu wakale wa MERA, a Collins Magalasi. Ndipo agwa nayo kale round yoyamba. Oweluza milandu a… ...
Kunali nkhanza pamene apolisi anapita kukagwila Mayi Martha Chizuma, Malawi24 yapeza choncho. Kupatula kuwakwenyakwenya, ati apolisi amauza a Chizuma kuti asamayankhule nawo chiyimile. Pa malipoti amene ayalidwa mu nyumba ya malamulo ndi a Kondwani Nankhumwa,… ...
In a shocking and deeply disturbing incident that unfolded in Mzimba district, Malawi, police have taken action by arresting a mob of twenty people who were involved in the harassment and assault of elderly women… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera wati a Malawi ochuluka akudzinyonga kamba ka mtima wa chifooko. Polankhula ku Mzuzu pamene anapita kukapemphera, a Chakwera ati a Malawi sakuchedwa kufooka mu nyengo zowawa zomwe akudutsa.… ...
Watsatira Winiko, naye kudzisiya. Amene anali mneneri wa chipani cha UTM, a Frank Mwenifumbo, atsanzika kwa mtsogoleri wa chipanichi, a Saulos Chilima. Malinga ndi chikalata chimene Malawi24 yaona, a Mwenifumbo ati iwo atula pansi udindo… ...
The Malawi Revenue Authority (MRA) says it will be operating from its newly built office for both passenger and commercial clearance at Mchinji-Mwami border starting on Monday the 21st November, 2022. The revenue collector announced… ...
Malawi has received a consignment of 2.9 million doses of Oral Cholera Vaccine (OCV) for a single dose reactive campaign to the Cholera outbreak in the country. The consignment arrives at a critical time as… ...
Photo by History in HD on Unsplash Politicians have never been immune to scandals. Bill Clinton and Monica Lewinsky were a part of the famous sex scandal, and Richard Nixon had to resign following the… ...
Mkulu woyang'anila bungwe loona za mphamvu la MERA, a Henry Kachaje auza a Malawi kuti asiye kaye zoyendayenda ndi cholinga chofuna kupulumutsa mafuta a galimoto. Polankhula pa msonkhano wa atolankhani umene bungwe lawo lachititsa mu… ...
A 35-year-old man identified as Siza Nyirenda has allegedly murdered his 15-year-old girlfriend, Maria Banda, and has cut off the penis of Maria’s 19-year-old alleged lover. According to Sub Inspector Gresham Ngwira, Public Relations Officer… ...
A unduna wa zamalimidwe atsutsa maripoti oti akathyali ena anawachenjeretsa ndalama zokwana 30 billion za fetereza otchipa. Malinga ndi maripoti amene atchuka, ati ma dobadoba ena a ku United Kingdom anatsekula mmaso boma la a… ...
Lying is a habit that can be developed over time, and oftentimes it's the result of gambling. While some people may think that lying is a minor issue, it can actually have some serious consequences… ...