As one way of containing the spread of the deadly Coronavirus, the Malawi government has scaled up joint border patrols involving the Malawi Defence Force (MDF), Police and Immigration in Mwanza . Confirming the development… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Mtolankhani wa wailesi ya Ufulu ku Chikwawa wamenyedwa ndi anthu omwe sakudziwika patangotha masiku angapo ataulutsa nkhani ya mnyamata wina yemwe akudwala nthenda ya COVID-19. Kumayambiliro asabata ino wailesi ya Ufulu inaulutsa nkhani yomwe mtolankhani… ...
Chiwelengero cha anthu omwe apezeka ndikachilombo ka Corona, komwe kakumayambitsa matenda a COVID-19 , chafika pa anthu makumi atatu ndi mphambu zitatu (33) tsopano. Izi zachitika patangodutsaso maola ochepa pomwe mlembi wamkulu mu unduna wa… ...
The Malawi Electoral Commission (MEC) has shifted the presentation of nomination papers for the forthcoming fresh presidential elections from this week to next month. Last month at a launch of an electoral calendar, MEC announced… ...
Chiwelengero cha anthu omwe apezeka ndi kachilombo ka Corona komwe kakumayambitsa matenda a Covid-19 m'dziko muno chafika pa anthu makumi awiri ndi mphambu zitatu (23) tsopano, ndipo asanu mwa iwo apezeka ndi kachilombola maola 24… ...
The MultiChoice Group has started rewarding both DStv and GOtv customers who are fully paid up on their subscriptions by automatically upgrading them to the next higher package at no extra cost. Confirming the development… ...
Ngati njira imodzi yochepetsera chiopsezo chanjala yadzaoneni makamaka kaamba kanthenda ya COVID-19, boma la Malawi lalengeza kuti liyamba kupereka thandizo kwa mabanja ovutikitsitsa m'mizinda yose yadziko lino. Izi ndimalingana ndichikalata chomwe boma latulutsa lamulungu pa… ...