Malawi24

Afa atamwa osadyera

Njonda ziwiri ku Manja munzinda wa Blantyre, zabzala chinangwa kamba kochita chibwana cha mchombo lende kukonkha chakumwa choyankhulitsa chizungu ku mimba kukulira malikhwelu. Malingana ndi wofalitsa nkhani ku polisi ya Soche, Aaron Chilala, Vincent Chotokoma… ...
Malawi24

M’njati wanjatwa!

Apolisi ku Chileka munzinda wa Blantyre, anjata wonyamula mfuti mzawo pomuganizira kuti adachita nsipu wamera mukhola pa mayi wina yemwe adatsekeledwa mchitokosi cha polisi ya Lunzu. Usiku wa Lachiwiri laliwisili, Victor Kachingwe, adachita madyera mphoto… ...