Mtsogoleri wakale wa dziko lino, Joyce Banda, walangiza mzika za dziko lino kusamala chimanga kamba ka njala yoopsa yomwe iyale mphasa chaka chino chifukwa cha kusintha kwa nyengo. A Banda ayankhula izi Lachitatu ku Domasi… ...
Articles By Peter Mavuto
Alimi m'dziko muno awalangiza kuti azibzala mbeu zosiyanasiyana ngati njira imodzi yothana ndi vuto losowa chakudya chokwanira komaso kusintha kwa nyengo. Mkulu wa Lilongwe District Agriculture Extension Coordinating Committee (DAECC) Akunsitu Kananji ndiye anayankhula izi… ...
Mabungwe a Rays of Hope, Save the Children ndi YODEP, alangiza alimi m'dziko muno kuti apewe kugulitsa zokolora zawo kwa ma Venda pa mitengo yosavomerezeka. Izi zayankhulidwa pomwe ma bungwewa akuchita chionetsero cha zaulimi mudzi… ...
Born in Malawi on 24 February 1934 at Kamoto Village, Traditional Authority (T/A) Chimaliro in Thyolo district, he came into power as a Joseph who saved his brothers and sisters including their families in Egypt… ...
Maiko ambiri a chigawo cha kummwera kwa Africa akupempha thandizo kuchokera ku maiko ena kamba kokhudzidwa kwambiri ndi mphepo ya El Nino yomwe inayambitsa chilala maikowa ndipo zadzetsa kukolora zochepa. Izi zadziwika pamene tsogoleri wa… ...
Mchitidwe okupha nsomba mosatsata malamulo ukuchulukira mnyanja ya Chilwa chifukwa cha kuchuluka kwa chiwerengero cha anthu amene amakhala mozungulira nyanjayi. Mkulu oyang'anira kaphedwe ka msomba m'boma la Zomba, Elliot Lungu wati kuchuluka kwa anthu kukukolezera… ...
Anthu okhala mma dera a Chiputula ndi Ching'ambo mu mzinda wa Mzuzu ali ndi nkhawa pa nkhani za mayendedwe kutsatira kuduka kwa mlatho umene umalumikizitsa ma derawa chifukwa cha mvura yamphamvu imene inagwa mu mzindawu.… ...
Malawi Police at Soche in Blantyre have arrested a man aged 41 for allegedly raping and impregnating his 14-year-old daughter. According to Soche Police Spokesperson, Aaron Chilala, the suspect has three children and the second… ...
Khonsolo ya boma la Thyolo yapanga lamulo loti eni minda ikuluikulu ya tiyi adzipereka msonkho ku khonsoloyi. Wapampando wa khonsoloyi, Rhustin Banda, ndiye watsimikiza za nkhaniyi. A Banda ati kwa nthawi yaitali eni mindayi samalipira… ...
Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga bambo Paul Mugawa a zaka 50 zakubadwa powaganizira kuti amagonana ndi mtsikana wa za 14. Mneneri wa apolisi ya Chileka, Jonathan Phillipo, wati a Mugawa anali pa… ...
Dziko la Malawi lapeza ndalama zokwana US$2 miliyoni (pafupipafupi 3.4 biliyoni Malawi Kwacha) kuchokera ku dziko la Israel kudzera mwa nzika za dziko lino zimene zikugwira ntchito m'dzikolo. Malinga ndi nduna ya zachuma a Simplex… ...
Mlembi wamkulu wa chipani cha UTM Patricia Kaliati wati mtsogoleri wachipanchi a Saulos Chilima ndiwo adzayimile mgwirizano wa Tonse pa zisankho za mtsogoleri wa dziko lino mu 2025. Chipani cha UTM chati mgwirizano wawo ndi… ...
A Undule Mwakasungula omwe ndi m’modzi mwa anthu amene amayankhulapo pa ndale ati a Peter Mutharika akuyenera aganize bwino pa lingalilo lawo lofuna kudzapikisana nawo pa mpando wa upulezidenti. A Mwakasungula ati ngakhale a Mutharika… ...
Akatswiri pa nkhani za umoyo ati kuchepa kwa kapezedwe ka njira za kulera komaso kusiyila sukulu pa njira ndi zina zimene zikuonjezera chiwerengero cha atsikana omwe akubereka asanafike zaka 18. Mkulu wa za umoyo ndi… ...
Apolisi m'boma la Rumphi akusunga mchitokosi wachiwiri kwa mphunzitsi wamkulu pa sukulu ya Mzungutwa a Wonderson Shaba a zaka 34 zakubadwa powaganizira kuti anagwililira mtsikana wa zaka 14. Mneneri wa apolisi m'boma la Rumphi, Noel… ...