
Anjatidwa kamba kozembetsa matumba 124 a chimanga ku ADMARC
Apolisi m'boma la Nkhotakota amanga mkulu wa za malonda ku Chidewe ADMARC, Patrick Duston wa zaka 35, pomuganizira kuti ndi amene anazembetsa matumba 124 achimanga a ndalama zomwana 7.3 miliyoni. Mneneri wa apolisi ya Nkhunga,… ...