Hudson Chamasowa
M’modzi mwa anthu opanga ndakatulo m’dziko muno a Hudson Chamasowa apempha boma kuti lilowelerepo pa ntchito yolimbikitsa ndikutukula luso la ulakatuli. Poyankhula ndi nyuzi ino, a Chamasowa anati boma pakali pano likulephera kuvomereza luso la… ...
Wapampando wa bungwe lomenyera ufulu wa anthu la Human Rights Defenders Coalition (HRDC) a Timothy Mtambo, alengeza kuti ayamba aimitsa kaye zionetsero pofuna kupereka mpata ku bwalo la milandu lomwe layamba kumva nkhani yokhudza zotsatira… ...