Arava Farm yomwe ndi imodzi mwa kampani zomwe zatenga a Malawi kukagwira ntchito mdziko la Israel, yati anthu mdziko muno asadere nkhawa za umoyo wa azibale awowa ponena kuti anthuwa akugwira ntchito mosangala kwambiri, ndipo… ...
Articles By Archangel Nzangaya
After decades of long journeys to fetch water from unsafe sources, people in Chiradzulu district can now afford a great sigh of relief as they now have access to clean and safe water through mechanized… ...
“Osewera tagwirizana kutenga zikho zonse,” mhuuu! Anakadziwa sanakayankhula, maloto a chumba enieni, chimanjamanja ikutuluka m'chakachi. Tsoka la mfutso lopita pa moto kawiri ndipo kupsa kwake ndi kwa chigumu, pansi ndi pa mwamba. Mukutipheranji? Walira movetsa… ...
Amid increased cases of unsafe abortion amongst girls and women in Malawi, a non-governmental organization, Nyale Institute, has encouraged authorities and relevant stakeholders to review the country’s sexual reproductive laws. This is according to Nyale… ...
Bungwe la Roads Fund Administration (RFA) lawopseza kuti oyendetsa galimoto omwe agwidwe akudutsa mokakamiza pa ma “tollgate” osalipira ndalama, alipira chindapusa cha ndalama yokwana 1 miliyoni kwacha. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe bungwe la… ...
Mtsikana wazaka 20 yemwe anamangidwa mu 2021 kamba kakupha “mwangozi” mwana wake wa chaka chimodzi ndi miyezi 9, lero ali ndi chimwemwe chodzadza tsaya pomwe wamasulidwa ndipo wauzidwa kuti asapalamuleso mlandu uli onse kwa chaka… ...
The University of Malawi Workers Trade Union (UWTU) has demanded clarification from the university's Registrar on why the Daily Subsistence Allowance (DSA) for workers in top grades has unjustifiably been increased more than the allowance… ...
Ma bishopu a mpingo wa Katolika pansi pa bungwe la Episcopal Conference of Malawi (ECM), ati zomwe alamula kuti a nsembe asamapeleke mdalitso uli onse kwa anthu okwatilana amuna kapena akazi okhaokha, sizikutanthauza kuti iwo… ...
Timu ya mpira wa miyendo ya Mighty Mukuru Wanderers, yati yavomeleza chilango chomwe yapatsidwa ndi bungwe la Football Association of Malawi (FAM) ndipo yati siyipangaso apilu. Izi zikudza pomwe komiti yomva ma apilu (appeal) ku… ...
Kuyelekeza ndi mchaka cha 2017 pomwe oyimba otchuka Dan Lufani anatchuka ndi zithuzi zomwe anaima ndi nkazi wake wake nthawi imeneyo ali oyembekezera, ulendo uno oyimbayu sanapangeso zakezi ndipo gulu latutumuka pomwe langouzidwa kuti kwabadwa… ...
The High Court in Lilongwe says it will make a ruling next week on Kondwani Nankhumwa's application which is requesting for the nullification of resolutions made at the Democratic Progressive Party (DPP) National Governing Council… ...
Ma bishopu a mpingo wa Katolika pansi pa bungwe lawo la Episcopal Conference of Malawi (ECM), ati zomwe wanena mtsogoleri wa mpingowu papa Francis sizikutanthauza kuti mpingowu waloleza maukwati a amuna kapena akazi okhaokha ndipo… ...
Bwalo lamilandu ku Mangochi lapeza olakwa m’neneri Christopher Phiri wa mpingo wa Supernatural Embassy pa mlandu oseweretsa malo obisika a mwana wawo wa mkazi zomwe akuti zinali ndi kuthekera koti anakagonana naye. Apolisi kumapeto kwa… ...
Anthu akudera la mfumu yaikulu Mtumbwinda m’boma la Machinga, akukhala mwa mantha kamba ka afisi olusa omwe akuti kumayambiliro a mwezi uno apha munthu m’modzi komaso loweluka lapitali avulazaso munthu wina. Yatsimikiza za nkhaniyi ndi… ...
Adindo awapempha kuti achite machawi kuthetsa nkangano omwe wafika posauzana m’mudzi mwa mfumu Limera m’boma la Machinga komwe anthu sakumwerana madzi, ndipo akumamenyana pali ponse pomwe angakumanepo kamba ka malo olima mpunga omwe akulimbirana. Tsamba… ...