
Mfumu yanjatidwa kamba kothetsela zilakolako zake pa mnzimayi wamisala
Mfumu Zatuwa ya m'boma la Kasungu yanjatidwa ndi a Polisi chifukwa choganiziridwa kuti yagwilirira mnzimayi wamisala m'munda wina wa chimanga muderalo. Malinga ndi m'neneri wa Polisi ku Kasungu Joseph Kachikho, mfumuyi inachita zoospazi m'mudzi mwa… ...