Malawians at a court in Chiradzulu
Kunali mkokekoke ndi maphokoso ochuluka kuchokera  kwa otsatila oganizilidwa milandu pamene oweruza milandu ku Chiradzulu anakana kupereka belo kwa anthu 15 omwe akuzengedwa milandu yakuba ndi kuononga katundu wa esiteti ya Mulli. Anthuwa adandaula kuti oweruza… ...
ACB and Ministry of Education have released a book for primary schools
Bungwe lothana ndi katangale la Anti-Corruption Bureau lakhazikitsa bukhu la tsopano lotchedwa "Anti-Corruption Source Book" lomwe lidzigwilisidwa ntchito ndi aphunzitsi a kupulaimale. Bukhuli lomwe alikhazikitsa dzulo ku Lilongwe cholinga chake ndi kuphunzitsa chikhalidwe, umunthu komanso… ...