Woman arrested for protesting against gender based violence


Malawi women

Police in Lilongwe this morning arrested a woman who was a part of the protests against gender based violence.

Reports indicate that the woman, Beatrice Mateyo, was arrested for carrying a placard which read ‘Kubadwa ndi nyini sitchimo. My pussy my pride’.

Protesters

Reports say that the police arrested her for carrying a placard that carried obscene words.

At the time of printing, her placard had caused a storm on social media with some coming to her defence while others have accused her of violating Malawi norms.

Malawians today took to the streets to protest against the spate of gender based violence.

Meanwhile, reports indicate that the woman has been released.

360 thoughts on “Woman arrested for protesting against gender based violence

  1. Sometimes I feel ashamed when I pass by market places and minbus stages some guys amatukwana kuti “Nyini ya Mako!” umenewo ndiulemu? ndeno azimayiwa they are trying to send a strong message to men that it’s their PRIDE thus they are asking us respect them. Tisiye kuwanyoza. Why is it that men are trying to ridicule chithu chomwe mazulo ake amachichitira kuchigwadira pasi kuchipempha. Ena osagona usiku kuyendayenda kuchifunafuna kupereka ngakhale makobi ambirimbiri. Stop insulting our women. Why insulting them because of their sex.
    Stop raping our women because if you rape them you are putting them to shame and you throwing out their PRIDE. They want keep it for a man who will marry or is married to them. Stop GBV

  2. Koma ngati ena akulonjezani Ndalama ndiye mwafikanazo penatu mukuswela ufulu makutu komaso maso atnu potionetsa tupt things l k that ngakhale mukt umeneoso ndi ufulu dont no sscc

  3. Needs a prison sentence to deter others carrying the same.Violence Against Women is defined as violent acts that are primarily or exclusively committed against women. Women are targeted expressly because they’re women (not because they possess a different sex organ).
    .
    I was surprised to see this placard happily carried and unashamedly displayed in this so-unpopular protest against Gender-based Violence. It beats me where it falls in the violence category because the distinction is very clear: #consented sex between #consenting adults (for whatever reason or purpose) is NOT an act of violence in any definition.
    .
    For my next point [to women], let me lay out the basic fact first: men (human beings with penises) are opportunistic by nature. Given the chance and guaranteed perpetual secrecy, most will bed your entire feminine circle (maybe excluding your senile grandmum).
    It should, therefore, not be surprising if they demand a carnal deed. They are simply taking the opportunity (your joblessness or lack of promotion) to satisfy their instincts. And they will use ANY means available (in this case power) to get into your pants.
    If they succeed,
    It means YOU are sooo weak to take a solid stand for what is honourable.
    It means YOU failed to maintain your dignity.
    It means YOU succumbed to YOUR desperation.
    It DOESN’T mean they hate you.
    It DOESN’T mean they are discriminating against you.
    It DOESN’T mean violence in any dictionary!
    .
    Therefore, if you have sex with your employers to get the job or a promotion (when you have 100% freedom, it means you are foolish. And it’ll be stupid to call it violence.
    .
    I do not imply that Violence Against Women is nonexistent. I simply don’t believe the above demonstrating placard reflected the real violence we (both men and women) should be protesting against.

  4. To say the truth. I do not see anything wrong with that placard. The problem is that, she wrote it in Chichewa. chinakakhala chizungu panalibe vuto. Do not judge this woman please. She just wanted to get attention of people about malpractice. Am preparing a case right now against government. Its an abuse to arrest her.

  5. eeeee! that was nuisance no way to say it publicly, who wants to hear such a vurgar languages, if its fine to u can u say it loud to the multitude and receive an applause? its not right to carry such a placard to the public ,they wud ve come up with another phenomenon!

  6. Mzimai changalama, uyenera ku mvera nyimbo ija yoti Naliyera- woimba Billy kaunda.
    Onse amene ayenda pa ndawala ija alibe azibambo. Wonse aja ndi mbeta kuteroku alibe amene amawamenya ku nyumba, ndipo akumufuna oti adziwamenya pakhomo koma sakupezeka amene akupezeka ndi omangowasisita, omangoseka mkazi akakana kuchapa zovala zao- sinanga ndi chibwezi nanga wa chbwez mpaka kumenya ayi.

  7. Anthufe ndife olemekezeka mmene Mulungu anatilenga, ndipo ndithu tinyadire chilengedwe chathu monga Munthu pa dziko lapansi lino. Ufulu wa Azimayi ndinso kusawachitira nkhanza, ndithu ngakhale buku lopatulika limati mkazi wako ndi thupi lako. Koma chinthu chimodzi Azimayi chonde tazilemekazani ndinu amene munatibereka anthufe, ndipo thupi lanu chonde ndinyumba yathu. Taonani ngakhale nyimbo zoyimbazi ndinu nokha mukupezeka kumavina kuonetsa malo obisika pomwe azibambo akuvala bwino zedi ngakhale kuti akhwefula tayang’anani amakhala atavala boxer, saonetsa matako ayi kapena katundu amene ayii. Kodi mwatani Azimayi chonde kubungwe lanuko muzitha kukambirana zimene mukuzichotsa nokha ulemu dziko lakutengani kuksandulani advertisement yovula zovala. Ineyo zimandwawa zedi chifukwa ndinu Amayi athu ku dziko kuno ndipo thupi lanu ndilolemekezeka koposa lathufe azibambo tikuuzeni poyera mosabisila. Tengelanikoni Chisilamu ngakhale kuti ineyo ndine mu khristu, koma asilamu amandisangalatsa kavalidwe kao. Chonde Chonde Chonde sinthani si ufulu umenewu chonde chonde.

  8. Osayiwala ngondya zinai,this freedom of speech and freedom of doing what you want it is bad to our nation,No matter what woman’s must always respect themselves so that men must learn to respect .But if you disrespect yourselves in doings alway this world will be pain for you,don’t forsake the word of God a woman was made for man,in so woman’s respect your husband so that they should love you.Now you are putting NYINI in public zikunthandauzanji, mwapepusa azimai onse m’Malawi chifukwa cha kupusa,this are the same woman’s who are arrogant and kamwa lao ndilowola mwalakwisa kumutusa ameneyo azimai ena a ngati iyeyo akanatengelapo chisanzo

  9. ….advanced idiots…. Release the lady… If she had expressed her thoughts (words) in English you wouldn’t have an issue with it…. Mentally chained idiots!!!!

  10. Angakhale yellow/red card imaperekedwa kwa amene wapanga foul even if mu pitch muli ma player 22 in total kkkkkk. Plz officers, get hold tight to tht woman ONLY kkkkkkk

  11. Ana akeso a mayiyu awerenga nawo zomwe analemba masteni awo, wat a mother kkkkkk,,,,,,,,let ha rot in jail. Freedom fighting has got its own dos n donts, if she cant keep within the bounds of reason, should feel the yammy yammy side of her nosense. Just like in a court of law, u cn never hear such profuse vulgarly vocabulary no matter how much profane stuff might b involved in that particular case(maliseche amalekezedwa). Get the point.

  12. That placard is just showing unger .. I think is good to deal with wants behind this protest that arresting such a poor soul fighting for what’s right..! Zikuoneka ngati zotukwana just because sees honest enough to say in public whats bothering wemen mma office mu..

    Its good amutulusa.
    Zolakwika ndizifukwa zomwe apangila protest zo osati the way of fighting it.. Maganizo anga.

    1. She is not a poor soul as you think, being a poor doesn’t mean you should not behave. Azimai ena ndiokhumudwa kwambiri ndi zimene. Wamva Priscar

  13. arrest?what for?the world is going to an end,remember the Bible says’matsiku osilidźa zobitsikà źiźuĺurika.Its time to open spiritual eyes

  14. pamenepa uwu mumati ufuluwa tikuugwirisa ntchito molakwika mpaka kulemba mau amenewo zowona malawi ukupita kuti mpaka kumatukwana mumsewu mwapadera ulemu upite kwa apolisi pogwira mai opanda mwambo ngati ameneyu

  15. pamenepa uwu mumati ufuluwa tikuugwirisa ntchito molakwika mpaka kulemba mau amenewo zowona malawi ukupita kuti mpaka kumatukwana mumsewu mwapadera ulemu upite kwa apolisi pogwira mai opanda mwambo ngati ameneyu

  16. There Is nothing wrong with the placard akanalemba kuti vagina sakanamangidwa. kutchula dzina la chiwalo sikulakwa koma kunyoza chiwalo chamunthu ndi kulakwa.chilankhulo chathu timachikana that’s why zikuoneka ngati watukwana let’s promote our language not this so called queens language. NO CASE.

  17. A police achita bwino kwamanga mayi ameneo ndipo amayenera kumanga gululonse lasimayi amanewa chifukwa akufuna kuononga dziko potengera chikhalidwe cha maiko ena kuno kwathu.

  18. and we call it a democratic country?? like really?y the hell wud she be arrested for saying it as it is?i thought in a democratic Nation we got a voice we need to be heard?Malawi is still way behind Democracy #MYOPINION….in as much as to say #Nyini sounds heavy and kinda insultive in a certain way but then wat do u xpect wen u gv them freedom of speech?do they have to gv it a certain name?how do they have to xpress themselves?

  19. Ngati Si tchimo mwalekeranji kupanga ma Demo muli mbulanda? Koma ndinu okwatiwa inu? kungozionongera mbiri azimai apa Malawi chikhalidwe mwasiya kuti? Zamanyazi kwambiri.

  20. analakwitsa nyini ndi chiwalo cholemekezeka its not proper to mention it anyhow.only health workers can mention it when on duty.tidziwe lero kuti nyini sitimaitchula paliponse its an offence ndizosiyana ndi mbolo

  21. If they new the meaning of gender I blv they would not do that nasty thing. Knowing what gender means they would vividly know what it means when we say gender based violence

    I blv the protest wasn’t for that of gender based violence, these are prostitutes.

    Gender based violence is not perceived in that stupid message they showed us Malawians.

    I suggest that who ever was involved in this protest, must be arrested, for they agreed as a group that whatever message they showed us was OK to showcase the violence of gender.

    Arrest them all and let them pay for that, may they can learn something.

    Ngati alipa ntchito yokhuzana ndiza gender awachose basi popeza kuti sakuziwa kalikonse kokhuzana ndi za gender

  22. Am happy to hear this. I even condemned early after that placard go viral on social media. How possible munthu wamkulu ngati ameneyu behaving like an animal? Am very thankful to the law enforcers to carry their duty responsibly

  23. Ku malawi tachulutsa kuyenda mu nsewu [protesting-]Opanda cholinga chenicheniNanu mabungwe mumationjezaKu ma radio stationku timuuthenga tosalongosoka essh!Tiyeni tizigwira ntchito tileke zomangoyenda Mabungwe limbikitsani anthu pa zokweza dzikoMaiwa sadachite izi mwa iwo oha ayi koma ngati gulu.

  24. MALAWI WALERO mpaka pamenepo apatu apolisi nawo angopezelapo podyela akangopeleka Ma alovele sibasi amutulutsa Koma mwin moyo akuona zonsezi masikuano anthu sakuopa kuntchula ziwalo zobisika or pa fb pompa zikuchitikaso kumango tukwana zonse zathupi mwamunthu kuziika poyela koma choti tidziwe chnchi si bwino kumatukwana Chikhalidwe chathu chilikuti Amalawi?

  25. Nothing wrong with that. It was hard hitting no holds barred. Let her be. Of course what makes a woman a woman and a man a man?

  26. Analakwitsa kulemba mchichewa chizungu chokha chinali chokwanira kuchizungu kulibe kutukwana koma kutchula,,,bwanji ku xul timatchula chilichonse pa biology popanda vuto koma kuti wina atchule mchichewa xul kutha basi

  27. Apatseni ufulu azimayi. Asiyeni azitukwana. Mesano mayiko omwe amatithandiza ife anthu amatukwanaso pa public? Ngati mukufuna ufa ndi ndiwo, nkhani imeneyo itayeni.

  28. They have rights to protest but mind your Ps and Qs when choosing what to write on the placards otherwise it’s gonna be like a joke to everyone and your voice will not be heard.

    1. kkkkkk koma man amalawi ndidzitsilu the fact is onse akumuikila kumbuyo mnkaziyu ndi mbalame chifukwa zomwe walemba hureyu ndi chifukwa chimene akupangila zionetselo its tottery different kkkkk man tell thise idiots to keep quite if they don’t have some thing to say

  29. Freedom. Free – dom wina akatanthauza ma words amenewa paokha paokha apeza kuti nd zisiru zikhale momasuka. Democracy. Demon – cracy: uwu ndi ulamuliro wa satan. Now ulamuliro omwe umayendesera boma la malawi sikuti anapanga amalawi. Kilipo komwe zidapangidwa ndicholinga chomulora satana kugwira ntchito zake muziko.

  30. Mmene zikuonekera zikukhala ngati m’mayi otukwanayo anangopezera mwai pa demo ya anthu olongosokawa koma ali othamangathamanga ngati m’mene amapezera mwai anzathu otolatola kukalowerera toyitoyi ya a ma taxi pomwe iwo sizikuwakhudza ndicholinga chofuna kukasolola.

  31. Men r being deeply abused by such runatics who call themselves women and lawmakers just smile about it and say “its unfounded”

  32. seems everybody was happy with that placard including the police cz the picture shows the woman carrying the placard and the police aside escorting, And somebody had to remind the police that obscene is not allowed and they had to come back to their senses and arrested the woman for few minutes just blind fold us.. i think this nation needs people who think people who use brains not antennas like grasshoppers to control and correct such languages before they are displayed in public.

  33. Much as I agree that the placard was bad, I disagree with the arrest. It is wrong and must not have happened. The setting is making the arrest a joke… You have to look at the context where that was done and in this case there is nothing to warrant her arrest.

  34. That’s malawi walero, tikapanda kuphunzra ntchito mayaz tiphunzre kutilemba ntchito mwat mutikwere Kaye amuna adishe Kaye, zimakhala choncho?

  35. My take is that the arrest is uncalled for. Bcoz when marching placards do change hands from one member to another

    They wud have just taken the placard and warn the marchers not to use such.

    1. Is this the the language which this time around can teach the youngsters to speak… It’s used to be a foul word my view is i think if she could have simplified it….it’s hitting hard while she may be right according to her experience anyway

    2. Hahaha my take is,every woman has it and it the wholesome creation now she has expressed it as a disability…..she has an element of psychiatric i rest my case

  36. Azimayi /atsikana dziwani chomwe muli a mabungwe amangokupusitsani mkazi wawo sangapange kunyumba kwao akungofuna kukugwiritsani ntchito iwo azilandira ndalama kuchokera kunja

  37. Thats bulshit mkazi ameneyo ndi opusa,ngati panali uthenga wabwino pazomwe analembazo sanayeneranso kulemba koma iyeyio anayenera kungovura mburanda kuti chomwe amanenacho anthu achizindikire nsanga. komanso apolisiwo amutengerenso ku zomba mento

  38. Mawuwa alakwika chifukwa choti alembedwa mchichewa KOMA akanati alembedwe mchingelezi ndikukhulupilila kuti sizikanafika pomangana komaso inu a Malawi24 simukanaika pa page panupa

  39. Mai amenei alibe UMUNTHU ndithu,inde kuli ufulu koma pamakhara marire ake.choncho abare ake,mamuna wake ndiso ana ake pokuva aziti amai anaremba chani pokayenda kumsewu???

  40. I have been traumatized and worried about my illness for 10years ,I was diagnosed with HIV virus and cancer this have been disturbing for long not until I recently saw a post about a Botswana man sharing testimony of how he was cured of HIV virus and his family,immediately I messaged him and asked him how he got the cured, and he told about the doctor who got him cured of the virus, so he gave me the doctor details then I contacted the doctor without hesitating,so I called him and doctor gave me some herbs which I used for some weeks after finishing it I went for a test as he told me to when the result came out it’s was negative was still doubting when the result came out I went to different hospitals for check ups and they found nothing. Now I’m free from all this deadly diseases, so if you know you have HIV virus and others diseases contact the doctor and he also on whatsapp Messenger with this number +2349069720659

  41. kkkk…tangokhululukirani bkoz some of those women were from #New_Dzawone_Bar ndiye mwina nayeso adachokela nawo komweko ndiye mwayiwo wumunthu ndi wuzimu mulibiretu…

  42. I’m lost indeed.. Kkkkk…. What’s wrong there by the woman? What is Nyini after all?? What language is that? And what’s wrong when someone pronounce it openly? Is Nyini an insult or a body organ? Such type of descence of avoiding calling Nyini publicly is what promotes Gender violence. Stop violence against women, then Nyini will not haunt you. I enjoy Nyini very much and I hate those who feign not enjoy it while at the time are masters of Gender Violence. Wake up!!!

  43. Kodi a police wo atapanga kafukufuku anapeza kuti amene analemba poster imeneyi ndi amene wamangidwayi? Mkuona kwanga ndikuona kuti panali a police ambili. Ndiye mwina poti kafuku fuku timvanso kuti ena amangidwa ndi nkhani yomweyi.Tikudziwa kuti chatchulidwacho ndi dzina lachiwalo chamunthu koma chikuyenela kutchulidwa mwa ulemu,nanga ana tsiku lina akadzatchula pa gulu tidzati chani.Eish Malawi akumila uyu.

  44. Mmmm angobwera ambuye msanga adzatiweluze tose wotsara adzatsala chifukwa yikuchimwa kulaura kuposa mwini mchimoyo oti ambiri mwa ife satananso akatiimba mlandu wakuti “BWANJI TIMACHIMWA KUPOSA IYE” Bale. Ndi mlongo Wanga dziyang’anire wekha coz masiku AMOYO uno atha wekha taona

  45. She went too far, the placard was wrongly packed, any way what massage was she trying to sent? That massage is a disgrace to womanhood! Sometimes its good to have limits when conveying massages! Shame.

    1. Everyone has a say as it is a world of democracy and I can like challenge u that she wasn’t wrong by doing that. If u ask me to justify this I can do that

    2. anazolowera kutsutsa zilizose awo alekeni,koditu fiti zimasowa ngati,zima talker nosence pa zinthu za serious,,,

  46. Our MPS,arresting is not a solution,other individuals are doing things for sheer ignorance,they need ur guidance,civic education rather than harrasing them

  47. Protesting against Gender-based Violence is not an offense, but it is impudent to protest in an indecent manner, especially anything to do with nudity and anything else that borders on nudity.

  48. I think this lady she not straight something wrong with her, maybe she is a prostitute, nzimayi waulemu wake sangapange zimenezi

  49. I used to cry thinking I would die of the HIV virus, I never knew there was a cure to HIV until I was completely cured from the virus by Dr Ikuku herbal medicine after suffering from the virus for over 7 years. Sometimes last year a lady posted on this page of how she was cured by this Dr Ikuku. At first I doubted her but I was convinced when I saw others the doctor has cured.I tried the herb and it worked on me. I can boldly say I am now negative after series of tests conducted by different doctors. If you are positive or have any disturbing sickness you can contact the doc now on call or Whatsapp +2348079062707

  50. At a very Rapid pace Malawi is becoming a demonic society.

    We are quick to protest but very slow to work our poverty out.

  51. Just Let her out of the custody when apregnant woman give birth she uses what is there acase the paralcard was just written to project their concern do not judge thats the God^s task not police.

  52. Illegal words? freedom of expression that’s when it comes in.Will you give her freedom back now do not be stupid by keeping here in your cells.

    1. Chi Pie shame too. That’s freedom of expression if u don’t know. The fact that the placard had used the vencular word that doesn’t mean u r breaking the law or whatever. Kma nothing is wrong with that

  53. Nothing wrong there mesa? it’s party of ladies. Have they arrested her bcuz of writing hers private party in Chichewa or what. Nanga amene amati khomo lachibelekelo why don’t they arrest them or anyone who callls or writes something that z on their body in Chichewa. Zamudulidwe etc….Am not saying she is right by writing that kma the police they are wrong with that.

  54. no law no sin .
    law placed is going to judge her we have morality laws in Malawi private parts are not allowed to be talked publicly its insulting others.

  55. Ngati pena azimai akumakumana ndinkhanza zina mwazifkwa ndizimenezo… wawonetsera kutukwana pagulu kodi ameneyu angalephere kutukwana mwamuna wake?….what ashame pliz!

  56. This is too much indeed! Zadutsa pa ufulu. Ana timawaletsa kutukwana, nanga akakufunsani pamenepo kuti amayi alemba kuti chani APA mungamuwelengere mwana wanu? Wanyamula poster imeneyi kukhala mkazi wanga sindingamulore kubwerera kunyumba kwanga coz ndiwochititsa manyazi. Nditha kungomuyimbira foni kuti akhale kumseu konko asabwerenso

  57. U should report fairly koz ve woman was not arrested for protesting against gender based violence , but for using illegal words

  58. mahule zintchito zawo kutukwana, munthu wa nzeru zoona ungalembe za uchitsilu ngati izo kumayenda nazo mu street!

  59. That’s what I thought too that anyone who started that no sense must be arrested! …
    Malawian is a well known respectful pple..
    All mayb we’re being under American colonial again?

    1. so in your country you don’t appreciates pipo who voice out when something is wrong,u shud try to understand what gender Based violence has done to women…think..

    2. R they violeting there Pusy r what? Why not just to speak what’s in there minds without insult,? Where’s our manners?,

    3. whats colonial?have we ever been in American “colonial”? please madam don’t disgrace your teachers here.That’s why that woman instead of using bloken English just used her mothers tongue Kubadwa ndi nyini sichifukwa..born with a pussy is no reason to be abused.

    4. Kuzolowera kutukwana waoneka choncho… I asked U that question becoz Americans don’t mind to insult …… We’re Malawian lets respect our tongue …. Don’t just follow everything…

    5. Some people are very happy to see that post written Nyini and they don’t even saw any problem about it …let me tell the ones you are happy for that post to stop calling your Mom Ma, Mom or Amayi instead u must call Nyini or Pussy coz it sounds good for you…what gender gender violence are u talking, where is our country going now ZAUGALU BASI NDE ANA TIZALANGIZA CHANI AKAMATINENA KUTI PANYINI PANU AMAYI ZAUMVE BASI MXM

    6. I think he who organized for the demonstrations should be cautioned because this is beyond ufulu, more over being a lady who wrote and carried such a placard, if it were a man I don’t know how far this could end.

    7. Tell them to even call there girlfriend’s or wife that name let’s c if they will not get a slap infont of everyone……. Phyllis Patricia Mwenda kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk..

    8. how brainwashed are we?the whites lied to us that a word said in vernacular is more obscene than the very same word said in English…kkkk how pathetic …cant imagine saying or speaking my language being an offence that can take me to prison…in American demonstrations against antabotion laws brought by Trump administration, women carried placards written “i own the pussy i make decisions”.

    9. Yes sis @ Mercy Phiri they must call there mom and wives even sisters Nyini come here pussy cook let see if they will be happy. ..we are not white we are black and our country got good example to other countries…so what is this now if our neighbours see that post …sitimavomereza zausiru ayi kumakhala ndi mphuziso kwa anaa …enanu zakusangalasani kumaona Nyini yamanu pa air choncho

    10. She was not calling her mom ,she was not calling anybody,she was simply demonistrating,she was neither naked nor nude,.come on dudes this is not a village..this is a nation .you cant arrest some one just because she used her language…

    11. Mmm yah mavuto simalilo okha ndithu aya ndimahvuto mavuto . Banda ase we are not whites if they do it in america I don’t think she was going to be in custody , I know Malawi as a well behaved country in Africa guys . mau ngati amenewa siopweka ndindu . @Banda if you want to do as whites do ends mumuseu ndiapongozi wako atavala kabudula wongopimba matako basi iweso uvale kabudulaso . olo mukhale pakhonde utavala pant iwe ndiapongozi ako ndiamai ako , tione kuti zitheka . zazungu zazungu guys chikhalidwe sichisinta ayi chifuka chakuzausilu. Sorry my chichewa is not that good

    12. Ok basii mama tiyeni tipume tione mphasa usiku wabwino azibale anga nonse mwapanga comment hv a lovely night…

    13. Palibe kugona lelo mama. zachitikazi zandinyasa. Maliseche a mzimayi ayenela kulemekezedwa. Amangidwe onse amene akhuzidwa ndi ziwoneselozo.

    14. we are not in the 90’s where by saying nyini was so hard…lets try to move with time saying nyini is the same kunena khomo la chibelero no difference in these days…back in school teachers would say that so i see nothing wrong..by the way what she did was freedom of expresion

    15. These conservatives dont understand here….the question is should we arrest anyone who says nyini?how many can we arrest?The real criminals are there in the town troubling us day in day out…these coward police are arresting a woman for a linguistic foul we havent even found substitute for…..in our Chichewa dictionary that word is found……if we continue victimising women like this we will be an asshore for a nation….Winiko went in town half naked nobody arrested him…Our own Vice president attended an event for action men..who wore pants

    16. only a cowered person will agree with mercy,you over looked to what these woman are fighting for but you chose to Blame these women for there writings…try to give credit for them,there fighting for millions of women

    17. Walakwitsa chan uyu? azimayi akumazijambura maliseche nkumatumizira zibwenzi zawo mapeto ake nkumayalukanso nde inu mukunena zongolemba

  60. all protesters who were part of the group including the police escort should be arrested because they did accept the placard

  61. Why not arresting the whole group? Because before they started their protest, the organizers were there,they could have seen this. It means every protester was happy with it.

    1. U mean the other demonstrators did not see what their friend was carrying? Was she demonstrating alone? Can u just see in the picture pls..

    2. chuluke chuluke ngwa njuchi umaloza yomwe yakuluma.she is arrested becoz of the offence she has commited.other protesters did not carry offensive materials thats y they were spared

  62. cz panalembedwa chichewa kumugwira koma pakanakhala chingelezi chokhacho ndikukhulupilira kuti sipanakakhala vuto kkkkkkkk malawi ufulu unachuluka

  63. I don’t see anything wrong with that placard what is vagina in Chichewa? And also a noun is a name of everything….ife timaphunzitsa life skills in chichewa zomwezo timakamba

    1. Bwana Edward do you use the same language in your house, before your mom and dad before your wife and children if not, then there is everything wrong with the placard.

    2. Koma aliyese akuziwa ndipo sizobisa kt that message on placard is original..if yuh do research sex workers are the leading group affected by GBV coz of ziwalo zawo nde elephele kuzitchula? Inu a Raphael mulibe ziwalo? Zilibe mayina and mmabuku sizilembedwa? Sizakakwike coz chinali chichewa cholembedwacho…We have seen our radios playing raw music ndikangat anayamba amanga DJ nde lero muzit am a savage coz I ve expressed what I feel towards that innocent woman? Nonse amanene mwapanga reply apa criticizing me muzifunse ngt kutchula kt mkono,mwendo,mbolo etc ndi kulakwisa!!!!

    3. This was a Gender Based Violence awareness campaign!
      Nyini, Mbolo ndi maina a ziwalo zathu, same as matako, mutu, mabere, miyendo, maso, makutu etc.
      Ndianthu angati pa Malawi amene samanenana kutchulana maina adziwalo?
      How about, why people don’t find these names outrageous??
      Amfumu Akwataine!
      Amfumu Akachinda Moto!
      Pastor Mbolo!
      Why are these names not outrageous?
      Anthu asanene chilungamo cha nkhani zalakwika? ?
      If it was a different campaign I would understand how outrageous that would sound. But this campaign had to express the feelings, of those women that feel their human rights and lives are violeted against.
      I think in that aspect it’s fair to say they haven’t done any wrong doing.

    4. A spiwe ndi anzanuwo, mental anamangira anthu ngati inu. Ataganiza mwa uchitsiru monga muchitiramo, zosatira zake sanaone chifukwa chovalira. Anayamba kuyenda chinochino pomanena kuti chilichonse ndi chiwalo basi.

    5. Iwe singini ndiye sukulu ndi culture susiyanitsa. Wat kind of a teacher are you? Teaching that in class of very young people. Wat future Malawi are you building? Don’t behav as if u are a Tabula laza.

    6. Sad ick we should promote culture and mind yuh am African teacher I should not brainwash kids nthawi imeneyo inadutsa #Raphael yemweyo ndi nzeru zake za ubusa azibisa kutchula ziwalo zake

    7. Raphael Chikaonda munapitako ku mental ku Zomba kukaona kodi?
      Inuyo ndi church cha katolika chokha chokhacho?
      Simunamve kuti kuli azibusa or Abambo a katolika ochita zachisembwere ndi Ana atsikana komanso anyamata omwe?

    8. Ngati munthu ukuvala chovala kubisa chiwalo chako it means sichofunika kuoneka kwa anthu ndie usango kamba ngati mulibe umunthu iyayi

    1. Major 1 ndiyenso ndani, ukuwona ngati iyenso angakuchitire chifundo iweyo ndiumphawi wako wakumatilirawo pangani zanu man.

    2. Jafali tambala nawenso ndiye kapolotu iwe ukundifunsa sukumuziwa iweyo major 1 kuti ndindani we clark some jokes here osamapanga za phwala ase

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading