
Fierce fire has gutted part of Carlsberg Malawi factory in the commercial city of Blantyre this afternoon, Malawi24 can report.

According to reports, two people have been injured following the incident at the Carlsberg brewery section.
The fire which is still raging has also destroyed property worth millions.
Authorities are yet to disclose the cause of the fire, but unconfirmed reports reveal the fire started when some technicians were working at the section near highly flammable chemicals.
The incident follows another inferno that razed down another part of the brewery section some months ago.
Carlsberg Malawi has been having maintenance works at the brewery section for a while now.
This is a developing story and Malawi24 will keep you updated.
Zayamba kulikuluko! Kenako mashabin onse kenako nyumbazosunga kachaso.
Lilongwe or Blantyre?
Anti azakala sober ntawi yambili
Midoli ili bho bho man
Tsoka mmtunda ndi nyanjaa kuti mapemphero ana amulungu akugwira ntchito,next week tipanga za timidoli,win komanso chimbuku
Tsoka mmtunda ndi nyanjaa kuti mapemphero ana amulungu akugwira ntchito,next week tipanga za timidoli,win komanso chimbuku
kwatsala company yophika mowa wakachaso chenjerani moto wukulowela komweko.
WAYASA NDI M’BALE NDI PIYO
Be aware with retretchment…
kaya a solver
No more “greens” how sad.
Ndichifukwa Pamafunika Insurance Kuti Zikabvuta Chonchi Itithandize Zachisoni Mzoti Ngozi Zina Timachita Chokonza Anthu Ogwila Nchito Pofuna Kubisa Zinthu Zina Komanso Kuti Ena Aoneke Olephela Achotsedwe Nchito Mulungu Alowelelepo Kuti Choonadi Chioneke
Satana wadandaula, Koma Yesu wakondwa chifukwa oledzela sadzalowa mu ufumu wa Mulungu
Dzilirireni nokha akumwanu. Afanta dzisangalalireni nokhanso
Omg…what will the nation do without booze!!!
I TNM malawi hv lost de way! Need special prayer
Bwana Wyt apatu zinthu sizinayende juice wathu mpaka kupsa chonchi bola ikadapsa factory yopanga frozzy
Kkkkk chipongwechi apanga ndawadziwa
Beers
Yoyoyoyoyo kanjani!! Mara utwala wami u safe?? Green wangayo ali pabwino? Eish abantu
Mmmmm kachikena?
Osapysa ku accounts bwanji
Thats the result of hiring semi-skilled labourers.
Sizachilendo …..we used fi ds scenario every wher n #Mw jxt recall..hw many bussnes sector wer burnt n 2016 -2017? Yatsala capital hill iyakenso kachikena kkkkk……#team™[email protected]
Kkkkk kubisa maumboni
Girini wapsyerera
mukafuna kuba dollar ndi so,osatibowa,,,
Its part of life, hospitals, markets, schools houses nd any other places can burn down at one point or the other. Its just a shame that some people might lose there jobs,
kkk,shame on dem or God has to hav mecy on dem?
God is Merciful at all times, nd to everyone regardless of our iniquities or what we for our daily livelihood.
God hates Beer thts y theres Helo of fire …ask urself y tht fire ddnt burn Coka Cola company?
John 2:1-11 -Jesus ChangesWater Into Wine- On the – Bible …
Amen, alcohol is wicked, let it all burn to the ground! @ Pius there are 2 types of wine in the Bible, wine is grape juice and is OK, but if you leave it long enough it turns alcoholic and then you mustn’t even look at it – see Proverbs 23 KJV towards the end to explain it. Jesus did NOT turn the water into alcoholic wine.
you Moussa pussy. there people working there. that Carlsberg company contributes handsomely to Malawi economy so what shit are you saying now?
Brewing& Bottling Group Limited (BBGL) they r 1 bt differ in production Machinery-Carlsberg~Coca-cola&MDL
Shame
Koma mwamva nawo??? Ndiye juice apezeka pamenepa?? Manzy Phiri
Thus too bad,,, something is hovering around in malawi. Day after day listening to unsung songs…… alowelerepo ambuyee
inakhala kuti ndi nkhokwe ya chimanga ndinakadandaula koma mowa aaaaa olo upse.
Bad news…. will it not cause unemployment?
Tasked company yo Ndlama zitupe kkkkkkkkk
AAA SHAME
Eshiiii
Dpp government
Idont kno wat to say.pitala waononga dziko langa
GOD he’s great good news
This Malawi should pray hard, I don’t know what is coming ahead. No new day in Malawi, every day is the same, accident day.
This Malawi should pray hard, I don’t know what is coming ahead. No new day in Malawi, every day is the same, accident day.
Not only malawi my bru, come to south africa, wierd things ar happening, Malawi is beta
No special,chill, grn,kuchkch,Stout, eeeesh bas matsire may sire
Mulungu si muthu,zinalembedwa bas nyumba ya machimo ngat imeneyo
Ndalama ndi zinazonse zopanda tchito koma mukanati athuafa ndiangati nanga avulala ndiangati mowo amawina kwambili angulazina. koma moyo sangula
Satana bwa?Nanga tidziti NDI Mulungu?
Popeza boma lathu ndilolephera kugula ma galimoto a ozimisa moto acompaniyi amayenera kukhala ndi galimoto yozimisa moto cause is a big companyshame
haaaaaaaaaaaa! mowa wanga ineeeee!
Modili ikwela ntengo
Aaah will the government say it’s opposition even there?
So sad.
So sad.
zosakhala bwino, takhazikitsani COI, kuti ifufuze chikumayamvitsa motowu coz sikoyamba, mwana ndi Carlsgate.
Bwanji kodi company yichokatuyo ndie timwa chani ife chibuku basi?
Timwa Chibuku basi
bolani ngati munaoderatu okwanira weekend imeneyi.sibwino kuti tikamwe nazo masese izi so sad
bolani ngati munaoderatu okwanira weekend imeneyi.sibwino kuti tikamwe nazo masese izi so sad
koma nde mbolatu….. Malawi osauka kaleyu
Zopandanchito zachitabwino amalawi , tayiwalachimene tilipadzikolapasipano
Mhu mumwa cani ku Malawiko mmmmm ndiyeno kachasu ayenda malonda.bad news.
Hope weekend programs are not affected….
Hahaha koma ,ok
Osadandaula froozy akupezeka.
Mulungu akuphulitsa malawi so bad chilichonse cikukhala changozi sorry
Are the government going to declare a state of emergency to take away citizens rights
Safety first safety always. Pepa chill ndi azibaleako. Zisasowetu zakumwa
Thats is so good. “Ine ndilibe pulobulemu”
I Thank God For That Ndipo anakangowotcheratu yoseyo coz miyambo 20 v 1 amati vinyo acita ciphwete cakumwa caukali cisokosa. wosocera nazo alibe nzeru. God Forbid.
Fire doesn’t always gut, you know? Zizungu zolowezazi penapake. Smh
Pray for Malawi
Chatsala ndichan kut tiziwe zot time it’s over,Malawi ulindimwai kut zizindikila ukuziona ndimaso osat kuchita kumva,zowawisa mmasiku otsiliza
zawo izo azitha omwsmowawo zaziii acitabóo
Iwe midoli nde chani
Good
Good ooooooo nooo even fanta is made there
again? …
Very sad
Tiyeni tiyankhule bwino kuli amalawi amene akugwira ntchito because of carlsberg, its a bad development to the nation.Akulipira misonkho yaikulu kudziko tiyeni tikhale ndi umunthu.
Dzopanda ntchito kumukweza satana pamwamba, mowa ndimunzu wa machimo.
Yehova wakankiza kutukwana nkumat sorry unali mowa
zoipa simowa okha ndizambiri
Ingosekani zimenezi nkusekulapo church apa.
Anthu ogwira ntchito kumeneko akumaba ndalama nkumaotcha dala cholinga azisokoneza umboni tizimwa chibuku basi
Better makosana zosadandaulisa
Zidakwa sory
Waiting for bash
ndizokumwa utalhuta nsima inu musadandaule koma akanati nkhokwe za chimanga ndie kunakakhala kulira mwana ndi mkulu yemwe masayang’ana nkhope
Mizimu ya Alubino ya kwiya,
Nde zanyanya2 kachikenaxo
Kodi Carlsberg Analikobe ¿ Mafana Akachasu Ife. Ndipo Simuzamvapo Kut Factory Ya Kachasu Yapsya!
mowa ovulala ndi opulumuka ndiungati pilizi
And its not only beers even fanta ali pa chiwopsezo
Yaphya carlsberg yokha?
Ma companeonse amowa ayake basi chibukuso iyake
athu salary izioneka zichitila
ziyake tilibe nazo kusowekela kuli konse
Hope Production Ya Weekend Inali Itatheka Kale, Otherwise Tivutika Weekend Imeneyi.
Mowa uthe basi
But don’t increase the price of beer
midori iyende malonda
Oopps my goodness, what’s went wrong with
Holy ghost motoo !
Carsberg the best beer in the world pepan kachaso aende malonda
Azimayi achangu: keep it up ma dona nonse
zatha izi agule zina machine wogula kamuzu aaaaaa
Izi ndiye zoyenera kuphyazo, iyaa
Sad
Zoononga moyo izo ngati Pitala mmene waonongera Malawi
what! here in zambia,its a city market burnt to ashes.wat is happening?
if you talk of merkets bro in malawi its almost an every year event
shaa Mpira timenya waulere basi
magetsi ake ndiomwewa ozimazimawa mpaka kuocha company so bad
Kachikenaso?
l’m sad
Yachita bwino
Sorry. Too bad We need development not such things……
Koma mowawo uli safe?
inenso nkhawa yanga ili pamenepo. koma mowawo sunapwetekeke?
kenako muyamba kuotcha zipatala
Anthu enanu mitu yanu simagwira hw can u enjoy thngz lyk this?
Mwqyatsansotu koma yaaaaaaa. Dzulo mwaponya nsembe ya Moyo lero mwaponya ya mowa….. Inu simudzathekanso basi… Devil playing with people (DPP)
koma timwa mawa admin? ;-(
What is hapening there? few months ago the same hapened
Kachiwiri
Winawake amawasaka
aaaa kachiwiri.. .nde akumaotcha dala2
holy gost fire
Ife tikumamwa midoli palibe chotidandaulitsa
Sichonchi mubale, anthu ena akulela ana chifukwa analembedwako ntchito, tikachuka malova more problems
zoonadi azimayiwa atiojeza akuotchera dala komabe tizikhapwilabe be
Kkkkkkk za satana iz azichta bwino
Fuck you. When saiy za satana what u mein
Zasatanadi Izi Iya.
Ndi za satana sakunama m’bale yu. Ka mowa nkachani nso apa
Za Muhammad ndi zhiti..?!!!!
Idzi ngakhale dzitayaka ine kusangalala kwambili. ndingalile ngati itapya nyumba ya Mulungu.
Jealas!! Bad mind
Jealas!! Bad mind
kunyasa ngati pepa sunday
mulungu wakoyo ndi chiseru.ife mai maria amatipatsa chikho chosefukira ndi carleberg.
Mowa ndi munzu wa machimo. idzi ngakhale dzhtapya dzilibe ntchito stupid. bola kumadandaula anzathu aluza miyoyo ku bingu stedium aja.
opepeza sky kumaona ngati heven.iwetu umadya maeravi.astraut,cosmonot.i love a twin earth. we quark an atom.we are makin an engine to work on anti-proton.
Musachite kuzilemba mavesi pa mphumi kuti anthu aziwe kuti ndinu opemphera, si mowa okha umene umabweresa machimo. Aliyense ali ndi zofooka zake.
STUPID MIND AGALU INU PALIBE ZODZILEMBASO MA VS PAMPHUMI MOWA NDI MUNZU WA MACHIMO, KUCHITASO KUUIKILA MOWA KUMBUYO.
what’s wrong with you people????? aliyense ali ndi ufulu wonena maganizo ake. ineso ndigomva chisoni kuti mwinadi ena avulala koma ngati zayaka opanda ovulala ineso ndikuti # praise de Lord!!!! zimowa zanuzo zikubwelesa mavuto ambiri ndipo ndikanakhala ngati ndine Mtsogoleli wa dziko choyamba ndikanaseka kampani imeneyi.
Gud news
Milliam amenewo ndiye mau. ngati dziko lapasi lavulidwa msalu muzu wa machimo ndiye ndi mowa. ngati satana wamanga maziko padziko lapasi ndi pachipanda basi. maukwati akutha, nyasi zose padziko la pasi pano kholo ndi mowa. anthu ambili tikalephela mayetso tsiku la chimalizilo ndikumapita ku ng’anjo ya moto mowa.
Akunama Jafali w anena zowona yathokhaladi Nyumba yopembedxera kt mkadandaule iya
Enawa akungotsutsa fukwa amamwa Koma akudxiwa kt ukunena zowona bro mumzu watchimo ndijang’ala kuchimake kwachiwerewere ndiakachamba ndizina zonyasa zimachitka Malo omwera mowa
Kuteteza ntchimo. koma mulungu akakanthadi. koma tidziwe kuti Mulengi alibe za nthabwala tsiku la chimalizo tikalila ndi kukukuta mano.
kkkk,shame on dem or God has to hav mecy on dem?,
KUKUONETSELANI MOTO PADZIKO LAPASI POMPANO KUTI MUDZIWE KUTI DZINTHUDZO DZACHABE NDIYE WANTHU SIMOSANKHANA KULILA MPAKA MAMINA KACHASO WAPYA. KUMVETSA CHISONI KWAMBILI.
Kkkkkkkkkkkkk hahahaha
Dzidakwa muli mmadzi
Chiukepo Chipofya uli madzi kkkkkkk
kkk malawi wavuta
Mowa uli safe koma, achina chill ndianzawo achina green?
Man ofunika kukasuzumirako fast!
ofunika kudusilako man!!
hahahahaha mmakwana guys
hahaha koma yeah
Sumweda eti, anyway umadula
Azimai ndiomwe akumaotcha calseberg cholinga azibambo tisiye kumwa mowa kut tizakhala panyumba
IZI OR ZIYAKA ADANDAULA NDI SATANA BASI
kkkkkkkkkkk koma
Good News.
Not good, it help alot, thru it many have smething, employmnt, beerbuznes, gvment tax etc
Auwa!! kanjani ? (goodnews)
Whu?
good news indeed…apeza china chopezera ndalama
U r fools