Breaking News: MCP keeps growing, Lilongwe Dep. Mayor defects from DPP to MCP


Lilongwe City Council Deputy Mayor Juliana Kaduya who was an active ruling Democratic Progressive Party (DPP) member has joined the main opposition Malawi Congress Party (MCP).

Kaduya announced his joining of MCP during a political rally currently underway in Malawi capital, Lilongwe.

Lilongwe
Chakwera welcoming Kaduya

According to MCP Secretary General Mkaka, Kaduya has been followed by other 60 members from DPP.

More to follow….

296 thoughts on “Breaking News: MCP keeps growing, Lilongwe Dep. Mayor defects from DPP to MCP

  1. Mwana onyoza kholo afe ndithu aliyese amene amanyoza MCP ndi ozungulira mutu chipani cha makolo makolo iwe basi dpp ngati mankhwala athonje koma munthu wa zelu aliku MCP tiyeni tisankhe bwino a malawi

  2. This human creature has all along been mcp, dont fool us,,, Dpp saw this from adistance thus she was banned from attending Dpp rallies..,, scrap ya munthu kulowa scrap ya chipani

  3. Who is fooling who ?
    Spreading wings in your own nest, you call it an achievement ?
    We win battles by putting boots on the enemies territory.

  4. Mac, what property did you have to attract confiscation?? Everything was agreed to be for Kamuzu. Accept change if you are indeed a civilized Malawian…

  5. Koma abale mpaka breaking news kankhani kake kameneka? Malawi 24, are you serious? Me thought you have brought news of the day but eeeish total trash. Your crew needs to be vigilant enough in sourcing news. osamangobweretsa nkhani zopanda mchere then you see Breaking News. kkkkkkkkkk

  6. Komanotu muzatipeza Ku DPP zipitani tinalibe nanu ntchito , mwachita bwino kuchoka.

  7. Tikumana 2019,tizaona ngati Mcp itazawine,koma ndichenjezeletu apa sibwino kuzataya nthawi ndi kucourt azanu akupitiliza kulamula zikoli.Muzaziona.Inu mungabwezele mcp mboma inu,aah mwachepa kwambiri.MUZAZIONA.

  8. huke waganyu wachita boo kuchoka amasokoneza a prezdent mutu amafuna azimufira nde walephela A muthalika ndi ozilesa musiyeni akachindise ku MCP ife a DPP maso pasogolo.osadanda ayi poti BIBLE limati zonse ndizachabe mlaliki (1 vesi 1-……)muwelenge nose zitsilu,makape,mazoba A MCP muuze achakwela akapitilize ubusa nkhosa zikudikila abusa

  9. Has not lost direction brother its MCP which has lost direction you shall see Your leader is cheating you the party has not changed its colour Muzalira

  10. Short word from me. Malawian sitichedwa kuyiwala+kugunata! Nthawi ya Kamudzu mumati anthu anaphedwa, chipani choipa ena ananthawiratu sakupezeka ku Malawi. Nthawi ya Bakili zoyankhula mbwe, anaba ndalama, ndiwabodza koma ena mwa inu mumafuna ayimenso. Nthawi ya Bingu nayenso anayesetsa. Azungu atakwiya ndikusiya kupereka chinthandizo Bingu wayipa! Kwazabweranso amayi Joice Banda(mayi wa mandasi but strong woman) kuzapanga devalue kwacha, ndikuzagulitsa ndege for chimanga ma cash gate mukati a Malawi nthungululululu kumasangalala. Kunonoloka ife! Bingu mulungu kudzamuchotsa mdziko nkumati bola ameneuja. Munatsankha Pro.Peter nkumati bola MCP.

    We Malawian we don’t know which direction to go and this is the serious diseases. We don’t love our country even those who are in leadership they are there to make their pocket fat. Unless we start loving our country then we will know the best party or person to rule us.

  11. if both the mayor and his deputy are MCP it means the entire executive of the government are lodgers of the city.alendo a MCP amenewa.akukhala pa rent mu city ya enuwake.muchokapo posachedwa rent

  12. Can someone tell me, ” from which party did Juliana Kaduya started his politics?”. If not in ” dpp”, then ” why are you wasting your voices praising such a person?”. Bcoz it tells you that, this person is acting like a ” sex-worker” who always busy with sex in exchange for ” money” and not for ” desires”. Wake up Malawians such people are like ” whores/ is’febe/ sex-workers” in our communities.

    1. You are the most Stupid person Malawi has ever had! Is that a comment from a normal person? Eeeeish zimakadeti zikulira eti? Sunati ndi Chipani chakocho cha zimbava! MCP wooooyeeee!!

    2. Robins John Banda, tell me something: ” have you ever tested ndalama za makhadi?”. The way how you defend your satanic party looks like muli mgulu la anthu olawa ndalama za makhadi, kapena amene munawatsogoza anzanu ku ng’ona.@#bcareful brother Dpp ndi boma basiiiiii.

  13. Which direction are talking about dude only the blind like you can’t see what Dpp is doing. Didn’t you hear about single digit hit on currency? Development is happening in the country everywhere. Anyone can join any party of his/her party so if one in Lilongwe joins mcp is not strange thing.come 2019 shall see who will be rulling Malawi

  14. Ut just shows the down fall of dpp hence the Malawi flag also shows upside down at Au hahahah , Malawian are tired with these crooks called dpp

    1. The upside-down placed MWian ⛳ simply displays the fall of the current govmt, remember last time the president of the same governing party did stuck right ↪ there ??????

  15. Had it bin that Malawi is conducting fair election, MCP would hav bin in power by now,but the way election are conducted more than 3days pple still voting, am not sure if MCP will going to make it come may 2019, pple are just voting ceremoniersilly, and the winner are bin identified b4 election takes place,

    1. But u must know that people they stl joining the rulng party dpp but evryday but we dont put them on media they know that wining s theres

    2. Nanga chasowa,wat you must politics is a bad game taonani mmene akusolorera ndalamamu azigogo anu mavuto kumudzi akusowa mankhwala mzipatala mu nthawi ya MCP zinachitikapo

    3. Peter kupha ma alubihno ndiye Iwe ukunena chani zaziii ndale zachikale basi zoyendela mtundu chimunthu chikukubelani inu ndikumachisapota

    4. Umbuli suposa poima pachulu nkumanena zakuphedwa kwa anthu ndi MCP,pomwe Dausi,Ntaba ali kumbali yo lamula.Awo ndiochepa chabe odziwika.Ndikukaika ngati Lazalo akukhudzidwa ,ndi kuzuza komwe kudachitika ndi MCP

    1. Chikumbumtima ndichomwe chidzaku pwetekani. Because you don’t have any control if MCP is to win. If God says yes, who can say no!!!!!. Let God, be God.

  16. This is an indication that the ruling party has lost direction. People have lost trust in this party, that’s why they are leaving the ruling party.
    With the coming of 50+1 system there will be no way this party to be in power again. Every Malawian now must come out in open to support MCP. I hope that the only hope which is remaining is in MCP.
    DPP must go now it has failed Malawians.

    1. Alubino mwayamba matama kkkkkkk but DPP will not loosing because of single bitch,,,,,,muzinamiza MCP singazalamulirenso mmalawi muno, wamva Napweri iwe

    2. Whether U want or no but but idont see any wind which iz to come and blow to remove dpp where it is now..mcp is acentral region party.

    3. Wiseman b like a human being, to born an albino its not a crime or that somebody should b afraid to expless his/her views, don’t insult here we r all human beings, we r all equal

    4. Is not about swearing other people on social media . it’s about teaching one another, give your on idea with strong sense being albino is nothing but human being.

    5. Wiseman King Nswatie, you are among terrorists, and your are not fit to be found in this forum. Here we are discussing issues and NOT attacking personalities of other people.
      You must know that am proud of who I am, and this is why am participating in these discussions freely without fear. Go and look again at your mirror and see if you are handsome. Believe me, you will cry for yourself for being looking like a unknown object.

    6. Mmm alimi ndi amene amavota, paja alimi akwiya, dpp can not win. Chimanga mk60/kg? To buy 2 bags of 23 – 21 + 04S a farmer must sell 10 bags of maize 50kgs weight. Amwene palibe mlimi amene angavotere dpp. Athu a mtown savota. Mavoti ali kumudzi, akutuluka dpp akudziwa chilungamo coz ndi athu a ndale amene amadziwa chomwe akuchita, ayiwonera patali.

    7. Chaima ur a liar,dpp will win with mudslide,wakwera yakuphwa ameneyo anong’oneza bondo pompano musiyeni,alira kuti chweeeeeee,bola mudakandiuza kuti ngwachigawo china kma central aaaah

    8. Ndale ndaleeeeeeeeeeeeeeezoooooo Kodi a McP muzapanga ziko lanulanu kapena ndalama zanuzanu analitu abusaaaa awa why asiya dora kuchepa hahahahhahhahahahah bolaso kuzavotela aja amatipasa ma 50 bah ajatu than mCP

  17. Which means mcp will have the same faces we know nothing won’t change coz we will the same prostitutes who always into money

  18. Why are pple joining an opposition party instead of a ruling? Nkuyesa ngati anthu akulowa MCP WO akanakhala ma apolitical prostitutes bwezi akulowa cholamula kuti uhulewo upindule koma why are they joining opposition koti kulibeko cash??? Watch out. MCP more fire!!!

    1. Mukunama akulu ndindani ananena kuti anatumilapo Mulungu sangatsogolere dziko. Ndi Mulungu yemweyo amene anamuuza kuti asiye apulumutse a Malawi Ku mikango yolusayi or ilibe mano

  19. Kuchoka chipani cholamura ndikukalowa chipani chotsutsa mmmmmm, wodziwa ndale pamenepo wangodziwilatu kuti penapake zinthu sizilibwino, ndiye poti kuvomeleza ndikuvuta tiyenazoni.

  20. mmm..ma cadet adamuthyola mphuno uja pomukayikira kuti amatumikira mcp..ngwanu kale..mwamuyiwala? Kkkk…uja ankati komwe wathawira sikukudziwika akuopa masapota a DPP atamuganizira kuti wavotera mayor kuti akhale wa mcp,pomwe iye ngwa DPP..nde mudziti wajoina? kkkkkk

  21. kkkkkkkkkkkk ndale sikusitha mpaka anthu kumatuluka muchipani cholamula kukakhala osusa kkkkkkk kufoooka kwa Dpp kukuonekera kokha

  22. kkkkkkkkkkkk ndale sikusitha mpaka anthu kumatuluka muchipani cholamula kukakhala osusa kkkkkkk kufoooka kwa Dpp kukuonekera kokha

  23. Munthu omvetsa chisoniyo olo ndiye bora akweni Ali ndi anthu owasatira izi NDA ayivkkkkkk mulira ulendo uno DPP woyeeeeer

    1. if ur father kills ur mother,then u stil love and support him because he nursed u to what u r 2day,is that fair? ur father illtreats ur mum by cashgating her financial resources and u still clap hands for him? as for me whether father or mother bt as long as they r villains,they r going 2 face my poison

  24. Kodi ngati anthu salowa mu chipani chà fuko angalowenso kuti?Mcp ndiye bomalo mdziko muno believe it or not the handsome man must rule to make everything handsome with his bold English like Barack Obama and thus Dr.Chakwera!

  25. Amaiwo apita kumene anachokela ndiye ayende bwino komabe alomwe alomwe nophia.DPP 2019 MPAKA 2024 KILILI < MCP asaaaaa koma amatituzuza bwanji.komans UTHENGA WAPADELA kwa MYPs apite kwa JOHN UGAPAKE TEMBO akamuuze za companstion koma boma lamalawi ai anal4 antchito aMCP NDI CICILIA KAZAMILA.

  26. zazii sindimayesa ngati watuluka ndi Peter muthalika kapena Henry mussa …..zoti hule ameneyo adali wa dpp ndikuyamba kumvako

  27. Next you will hear that Kaliati, Vuwa, Dausi, Chilima, Obama Chiumia, Atupele & Getrude Muthalika have also joined MCP

    1. Jst know that to spy much.hehehehehe u dont know dpp techniques.Ask Tembo about Bakili.It was dpp move and now muli mwetumwetu a mcp,more and more are to come so as mcp is severely milked.

    2. Simeon Chimbiya,khulupilirani ndithu palibe za u spy apa,ndikutha ndithu kwa dpp uku.Tikamayandikira chisankho tiwona zambiri.Ambiriwa akungodikira kuti amalize kudyelera ma positions awo e.g ma ministers.It’s true that Bakili had techniques but not this visionless man.

    3. Mbendela ya malawi yatembenuzidwa ku nsokhano wa united nation yayamba ndi gilini mmalo mwa bulaki (end of the biggining)

    4. Mcp hmmm mwina chitakhala chipani china koma za dpp nonse mumaziwa izawina ndipo mosavutikanso mukamapanganso matukutuku tikakuyikàni pa #3 ngati pp mu 2014

  28. He do right to fulfil his freedom to join any party he want,people are coming and going but still the party remain strong.

  29. ndiye mukuona ngat DPP ingathe chfukwa cha hule watulukayo if you think so mukunamizana kwambili we will read ths country kupitilira 2019 zikumuwawa akakolope nyanja

  30. By the way on which party’s ticket did she win her councillorship? If independent, no problem. If DPP, she has made a monumental decision.

    1. No. She is not. She has simply exercised one of her freedoms, ie, freedom to right of association. It says any person is free to join or leave a group, inu ustupid wake uli pati?

Comments are closed.

Discover more from Malawi 24

Subscribe now to keep reading and get access to the full archive.

Continue reading