Police at Ndirande Township in Blantyre city have arrested a 37 year-old man for being found with Indian hemp locally known as “Chamba”.
According to police, the suspect Francis Khoza was arrested after he was found with Indian hemp weighing 300 kgs in a vehicle registration number KU 1751 on Thursday.

Confirming to Malawi24, Blantyre police deputy spokesperson Andrew Mayawo said the officers had a tip about the suspect who was packing the Indian hemp to sell it outside the city.
“The suspect was packing the illegal stuff at Makata and people of goodwill tipped the police who managed to stop his vehicle when he was about to leave Blantyre,” said Mayawo.
Mayawo added that the police have since sent the Indian hemp to Bvumbwe Research station as part of investigations on the matter.
The suspect comes from Mataka village, in Blantyre and he is yet to appear in court.
99 thoughts on “Chamba lands Ndirande dealer in cooler”
Comments are closed.

Kkkkkkkkkkkkk chamba ndi deal koma ukakodwa
ndi mbola
Apolice athu uchita kugundika ngati zoona onani uniform yangati chamba cha Nkhotakota
Am a buyer aliyese amene ali mlimi wa chamba i buy dont wory azanga market itsegulidwa pa 2july nkhotakota
a chana inu osamaga a cushgate
dis is bullshit!kumanga munthu cifukwa ca chamba, inu mmafuna aziba mmesa achimata ambiri akusowa tchito cifukwa cha ndyelalanulo,mukagwila wogulasa chamba nde mmanews ndi maradio kulengeza pamene mukulephela kuthana mbava/zigawenga cfukwa choti mumawabweleka nokha mfutizo?
Nyonyonyo Haigrade Dukse Gangsta sanalakwe uyu
Haha haha Ine nkhani zimenezi ndinasiya kuyankhila . Zimandikwiyisa kwambiri . Ndimawopa day ina nzayankhula mosakhala bwino
Haha..I know the feeling.instead of focusing on albino killings n sht..
Eti man . Kaya anamvapo kuti zoti wina wafa akusuta chamba
hahaha..Never
Za dziko ndi chocho palibe wabwino poti apolisi akugulisa chambaso ok
Why arrest innocent people? The man didn’t create the plant.
Why the police contineu arresting good pipo, like this chamba saller?, onbehalf of arresting those who are now killing innocent pipo/like albinos? Apolice aku malawi ndinu mbuzi kwambili mukummanga opezeka ndi chamba? Okupha albono ndemukumawasiya poti #4million?
Kkkkkkkk
Chamba chili ndi ndalama kuposa fodya aliyese tsono, mukumangiranji munthu poti iye amafuna ndalama zozithandizila pa moyo wake.kodi mudzamvomeleza liti ulimi wachambau? tatiyeni amalawi tizilima ulimi woti tizipeza ndalama osat uwu amangotibela azunguwa.