Chamba lands Ndirande dealer in cooler

Advertisement
Malawi police

Police at Ndirande Township in Blantyre city have arrested a 37 year-old man for being found with Indian hemp locally known as “Chamba”.

According to police, the suspect Francis Khoza was arrested after he was found with Indian hemp weighing 300 kgs in a vehicle registration number KU 1751 on Thursday.

police malawi
Police officers net trader. (Library)

Confirming to Malawi24, Blantyre police deputy spokesperson Andrew Mayawo said the officers had a tip about the suspect who was packing the Indian hemp to sell it outside the city.

“The suspect was packing the illegal stuff at Makata and people of goodwill tipped the police who managed to stop his vehicle when he was about to leave Blantyre,” said Mayawo.

Mayawo added that the police have since sent the Indian hemp to Bvumbwe Research station as part of investigations on the matter.

The suspect comes from Mataka village, in Blantyre and he is yet to appear in court.

Advertisement

99 Comments

  1. Kkkkkkkkkkkkk chamba ndi deal koma ukakodwa
    ndi mbola

  2. dis is bullshit!kumanga munthu cifukwa ca chamba, inu mmafuna aziba mmesa achimata ambiri akusowa tchito cifukwa cha ndyelalanulo,mukagwila wogulasa chamba nde mmanews ndi maradio kulengeza pamene mukulephela kuthana mbava/zigawenga cfukwa choti mumawabweleka nokha mfutizo?

  3. Why the police contineu arresting good pipo, like this chamba saller?, onbehalf of arresting those who are now killing innocent pipo/like albinos? Apolice aku malawi ndinu mbuzi kwambili mukummanga opezeka ndi chamba? Okupha albono ndemukumawasiya poti #4million?

  4. Chamba chili ndi ndalama kuposa fodya aliyese tsono, mukumangiranji munthu poti iye amafuna ndalama zozithandizila pa moyo wake.kodi mudzamvomeleza liti ulimi wachambau? tatiyeni amalawi tizilima ulimi woti tizipeza ndalama osat uwu amangotibela azunguwa.

  5. It’s Healing Of The Nation Don’t Criticise It U Are Failing To Catch Di Thieves and Criminals Bt Rush On Useless Things DemtBlust Jah Will Arrest U Too

  6. Eeeeeeeeeh bwanjiso mwina anakanika kukukongozani mesa ndiamene mumakonda kusuta chamba inu bwenzi tikukambapa mwina anagawana kale chambacho kkkkkkk aaaaah

  7. Eeeeeeeeeh bwanjiso mwina anakanika kukukongozani mesa ndiamene mumakonda kusuta chamba inu bwenzi tikukambapa mwina anagawana kale chambacho kkkkkkk aaaaah

  8. kkk ndirande sazatheka !!! Thumb up my fellow ndirandians ku makata,safarao,mapulot,newlines,malaysia,nyambadwe,majiga,mpembu gamulani and many more

  9. It is shame to see the police arresting one found in possession of Indian hemp setting free one found in possession of bones of an Albino….that’s not fair!….or maybe am missing something on indian hemp,I ever since I was born,have never heard of any death caused by marijuana…but look at those u setting free,they’re taking the life of fellow. humans…Wise up and free everyone found in possession of MARIJUANA

  10. ku malawi kuno umphawi uzatha pokhapokha atayamba kumalowa ma bussines obweresa ndalama. Chamba sikusuta kokha ma products ambiri omwe timapanga import ndiopangidwa from chamba

  11. ku malawi kuno umphawi uzatha pokhapokha atayamba kumalowa ma bussines obweresa ndalama. Chamba sikusuta kokha ma products ambiri omwe timapanga import ndiopangidwa from chamba

  12. We can’t success if you still doing like that smuggling ndiyomwe ingathandize kuti dziko lathu anthu azinva kukoma koma ñgati ndi choncho tizakhala ovutika mpàka kale anzathu mmaiko mwao anadalisidwa ndizàchilengedwe zomwe zimawabweĺeseĺa chuma komwe kwathu kuno ayi ndiye ngati wina akuźilimbiķila mwaiye yekha mukufuña mumubwezelese m’buyo eish my nyasaland wañtasadi ndi ntima omwe

  13. We can’t success if you still doing like that smuggling ndiyomwe ingathandize kuti dziko lathu anthu azinva kukoma koma ñgati ndi choncho tizakhala ovutika mpàka kale anzathu mmaiko mwao anadalisidwa ndizàchilengedwe zomwe zimawabweĺeseĺa chuma komwe kwathu kuno ayi ndiye ngati wina akuźilimbiķila mwaiye yekha mukufuña mumubwezelese m’buyo eish my nyasaland wañtasadi ndi ntima omwe

  14. Chamba Mmalawi Muno Chidayamba Kalekale Kusutidwa Mwagwila Yekhayu Bwanji? Kalimbanen Ndi Opha Albino Uko Ameneo Akugulitsa Chilengedwe

  15. Chamba Mmalawi Muno Chidayamba Kalekale Kusutidwa Mwagwila Yekhayu Bwanji? Kalimbanen Ndi Opha Albino Uko Ameneo Akugulitsa Chilengedwe

  16. Kusowa tchito basi koma tikaimba foni kuti okuba kuno ndie mumabwera akubao ataba atapita kale Kenako kuzamafutsa mafutso a tchayina.

  17. Kusowa tchito basi koma tikaimba foni kuti okuba kuno ndie mumabwera akubao ataba atapita kale Kenako kuzamafutsa mafutso a tchayina.

  18. koma apolice akumalawi kukonda katangale kwambili alimbana ndi munthu wa chamba moti azilimba ndi anthu amene akupha alubino koma pa nkhani ya ndalama eeeeeeee ndi chifukwa dziko lamalawi ndi yosauka sizachitaso bwino ayi

  19. Ogwirawo ndi mbuzi za athu inu chomwe mumabandacho mumatenga kt?kungokhala ndi umoyo wa umbava musabisetu china kt muzisuta muzalangidwa mulungu ali nanunanu

  20. Oky chabwino tamva koma funso langa kwa inu apolice bwanji mukulimbana ndi ogulitsa bwanji osathana ndiyamene akulimawo bwanji? pamene kukufesedwa njeleko mukuziwako zachinyengo basi tiziti mukugwira ntchito bwino muthana nazo bwanji zimenezi pamene njele zake zikufesedwa mom’muno ndipo mukuziwako. mbola imeneyo malawi police is poor

  21. analima monga njira yopezera ndalama zosamalilira banja lake akakagulisa kuma company omwe amapangira mankhwala a asima kukana kukaba za anthu ena kapena kuwoongera bongo la munthu wina, mwasiya mbav

  22. Demeti mumathamangila patinkhani ting’ono ting’ono koma akati akuba amfuti kuno ulendo okalowa m’bulangete nkonono ngati usiku…….koma masana #u_alwez_piss_me_off u akapokola

Comments are closed.