Police in Ntcheu district have arrested three men suspected of killing Fletcher Masina, a 45-year-old man with albinism, last Wednesday.
Ntcheu Police spokesperson Gift Matewere said yesterday the three were arrested after the law enforcers were tipped off about them.
He identified the suspects as Jussab Saiton, 36, of Zintambira Village, Traditional Authority (T/A) Chakhumbira in Ntcheu, Dou Mkwaila, 49, and Francisco Kamtsimtsi, 40, both from Phumula Village, T/A Kachindamoto in Dedza.
“The three suspects have been charged with murder. However, investigations are still underway,” said Matewere.
The murder of Masina occurred two days before Parliamentarians provided their suggestions on dealing with killings, abductions and exhumation of graves of people with albinism.
160 thoughts on “Albino killers arrested in Ntcheu”
Comments are closed.

Ndigwirizane ndi Arabi wa Leverpool sukunama,kodi chiyambireni cha nkhaniyi Ngati Boma palokha lachitapo chani? Ndipo an2wa amawatulusa pa bail komaso akulephera kuwapana kuti aulure za misika yao,Y? Akuopa kutchulidwamo akuluakulu a maudindo. Komaso malamulo akuno alibe mphamvu nde ife amene zikutikhuza tapanga malamulo athu ongogwirizira podiklira boma kuti likazapanga awo tizasiya ndipo malamulo ali motere:
Yemwe apezeke ndi mlandu wa izi aphedwe ndi kumuotcha
Ngati anamangidwa ndipo watuluka pa bail ayenera kuphedwaso
A malawi tisapusisidwe malondawa Boma likuziwapo kanthu ndipo ena mwa anthuwa ali mu gulu lomwelo nde olo pachedwe ZIZAULULIKA
Im very very disappointed with them let them vanish in thin air how can one think the way of dwindling poverty by killing an innosent person like dat please please we dnt wont to see them in our clean society again even if u can find them not guity but we r not ready to see them again find them a place to live not in our society we not
No security in Malawi why mr President
Eti chapikane kuti walamwile yaka nsano (5) kukaidi,kaneko kwakoposya.Ajimanjaji nambo kwajocha moto. Umi wa mundu ngawa kutenda geni.Yachanasa
Nawonso aphedwe amve ku wawa mene anamvera anzawo
Naonso aphedwe kukhala albino kusabweletse kulira pakati pathu
They deserve death by hanging….heartless idiots.
izi zafika popwetekesa mutu ndipolilisa apezeredwe chilango chenicheni chokhwima omwe akupanga mchitidwe umenewu
Opha nzake aphedwe!!
apolic amakonda kumanga anthu osalakwa,nanga olakwawa atani nawo? tikuonani kupusa kwanu apolic
Please please Malawians we known as peace loving people stop malpractice of killing our fellow humans,they are like any of us I beg I beg
iwo tsakufuna malbino mungowadula zokozelazo kuti nawotso atsabeleke albino sinanga amawachatsa koma chomwe tingaziwe ndi anthu ngati ife tomwe
Yawiniko Ian basi
So please don’t arest them coz the can’t leave there system of kill the abnal people the best solution is when u find them burn then or kill them as hw they kill the abnal mukuwatsekela mukundamusewu with ur demonstration kuimba nyimbo concerning abnal killings coz u wasting your time in doing that if caught the suspect burn or kill him/her end wy government there ar not seting the strong rule on that issues of kill the abnal please malawi work up we ar losing they of lnnocent people coz of those stupid people u malawians end the government ur a watching of that my Lord our God do something Amen
Ok