
Awanjata akusakasaka msika wa Nyanga ya Njovu
Apolisi m'boma la Nsanje atsekera matate atatu mchitolokosi atapezeka ndi Nyanga ya Njovu yomwe anatangwanika kutsatsa kufuna kupeza msika. Malinga ndi oyankhulira polisi m'bomali, a Agnese Zalakoma, omwe atsimikiza za nkhaniyi, atatuwa amangidwa nzika zakufuna… ...