Dan - Lu

Dan Lu watulutsidwa pa belo

Woyimba Dan Lu yemwe anawona ngati ku maloto pomwe anathilidwa dzingwe Lachiwiri munzinda wa Lilongwe, tsopano watulutsidwa pa belo. Posatengera kugundika kwake potulutsa nyimbo zochemelera boma la MCP, apolisi adanjata Dan Lu pomuganizira kuti wavulaza… ...
Dan - Lu

Kumenya kugwetsa!

Oimba odziwika bwino m'dziko muno, Dan Lu, yemwenso pakatipa wakhala akuyimba nyimbo zotamanda mtsogoleri wa chipani cha Malawi Congress (MCP), Lazarus Chakwera, wakwidzingidwa ndi apolisi masana a lero ku Lilongwe. Wachiwiri kwa ofalitsa nkhani ku… ...
Saulos Chilima - Lazarus chakwera

Ndinali mboni – JB

Mtsogoleri wakale wa dziko lino, Joyce Banda wati pa mgwirizano wa Tonse Alliance, iwo adali mboni pamene mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera ndi wachiwiri wawo wakale malemu Saulos Klaus Chilima amagwirizana kuti aliyense adzalamulira… ...