![Timothy Mtambo Malawi](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2024/04/Timothy-Mtambo-e1714217248986-235x176.jpg)
Ine ndiye Mose ine – watero Timothy Mtambo
Mudziwitseni Phungu Joseph Nkasa kuti analakwitsa. Mose wa lero ati sanali Mutharika, koma ndi a Timothy Mtambo. Atero eniake pomwe anapangitsa msonkhano wa atolankhani lero pofuna kukumbutsa kuti akadalipo. A Mtambo amene adachita chete pomwe… ...