![](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2022/12/Peter-Mutharika-Malawi-235x176.jpg)
Wayamba kampeni Mutharika, ali pa Njamba mawa lino
Mtsogoleri wa chipani cha DPP, a Peter Mutharika amene owakonda amangoti APM, akuyembekezereka kugwedeza mzinda wa Blantyre mawa lino pa 12 May. A Mutharika amene akhala nthawi osachititsa msonkhano wandale alengeza kuti akhala pa Njamba… ...