Mudziwitseni Phungu Joseph Nkasa kuti analakwitsa. Mose wa lero ati sanali Mutharika, koma ndi a Timothy Mtambo. Atero eniake pomwe anapangitsa msonkhano wa atolankhani lero pofuna kukumbutsa kuti akadalipo. A Mtambo amene adachita chete pomwe… ...
Articles By Mike J. Kangwele
Kokapumira ndi kumwamba basi. Patangotha ma ola bungwe la Blantyre Water Board litalengeza kuti lakweza madzi ndinso kampani ya Illovo italengeza kuti shuga wake yakweza, nayo kampani ya Salima Sugar yalowa m'bwalo pofuna kuonetsetsa kuti… ...
Kampani yopanga Shuga ya Illovo yalengeza kuti tsopano yakweza mitengo ya shuga wake amene sakupezeka molongosoka pa msika. Mu chikalata chimene kampaniyi yatulutsa, iyo yati kuyambira lolemba pa 22 April, ikhala ikukweza mitengo ya shuga.… ...
Ngati simufa ndi njala, ndiye mwina ludzu kapena kolera zitha kukuphani. A bungwe la Blantyre Water Board alengeza kuti madzi awo akwera mtengo. Mu chikalata chimene bungweli latulutsa, a boma tsopano awapatsa chilolezo choti madzi… ...
Uja anati menya galu kuti udziwe mbuye wake n'kutheka adalinga izi. Patangotha maola ochepa boma litatafulira boma la Amereka kamba koletsa anthu ena kupita ku dzikolo kamba ka katangale, naye tate wawo Chakwera wayankhulapo. Iye… ...
Ngati sanapiteko ndi komwe ndiye nyimbo ya Buffalo Soldier ya a Gidess Chalamanda asiya kumvera. Koma ngati anapondako kale ati asazabwelerekonso. Dziko la United States of America lalengeza kuti ena mwa adindo a dziko lino… ...
Inu nonse amene a Peter Mutharika simukuwafuna, yang'anani kumbali. Nonse aja olemba kuti "APM my vote", senderani chifupi. A Mutharika lero abwerezanso kuti chaka cha mawa akubwelera ku Sanjika. Mtsogoleri wa chipani chotsutsa cha DPP… ...
Nkhondo ya pa chiweniweni ya ku chipani chotsutsa cha DPP ikupitilira, tsopano akufuna kulikhirana ku malamulo a dziko. A Welani Chilenga amene anathotholedwa mu chipani limodzi ndi a Nankhumwa ati nkhalamba zisamayimire nawo pa zisankho.… ...
…Nigerian-Malawian woman married to a Pastor at the centre Details have started emerging of the elaborate doctoral scam that awarded honorary degrees to musician Patience Namadingo and his brothers in arms: Pemphero Mphande and… ...
…adds Mr Namadingo and Karim in the mix …Nigerian woman attributed with scamming Malawian ‘celebrities’ for 10 million Kwacha per PhD The University of South Africa (UNISA) has formally denied ever awarding any Malawian a… ...
Uja amatamika ndi za mafuta ngambwi ngambwi ali kuti? Chifukwa tsopano akuyenera kupepesa a Malawi, azingoyenda ali werawera. Mkulu wa bungwe la MERA a Henry Kachaje ati za mafuta ngambwi ngambwi ndi zoduka mutu, posachedwapa… ...
Ngati a Peter Mutharika amayesa kuti akadutsa moyela ku convention yawo, apa ndiye aganize kawiri. A Kondwani Nankhumwa sali mocheza ndipo ati akawaswa a Mutharika. Malinga ndi wailesi ya Zodiak, a Nankhumwa ati iwo sabwelera… ...
Mukamva ena akupitirira kunena kuti agona pa filling station chifukwa amasaka mafuta, adziweni ndi opanda chilungamo chabe. Mafuta analonjezedwa kufika lero aja tsopano afika. Ngambwi ngambwi, a Chakwera sakucheza. Patatha sabata a Malawi atazunzika ndi… ...
Mizere yonse mukuyionayi, ati mukuyiona komaliza. Kuyambira lolemba lomweli ili, mafuta akhala paliponse moti malo omwetsera mafuta azichita kuyitanira anthu. Atelo ndi a boma. Malinga ndi mlangizi wa a Chakwera a Ephraim Chibvunde, mafuta osowa… ...
Olira samugwira pakamwa ndipo mneneri wakale wa chipani chotsutsa cha DPP, a Nicholas Dausi, walira mokweza pa mwambo wa maliro wa a John Tembo. Poyankhula pa bwalo la za masewero la Dedza pamene amaimilira anzawo… ...