water tap
Ngati simufa ndi njala, ndiye mwina ludzu kapena kolera zitha kukuphani. A bungwe la Blantyre Water Board alengeza kuti madzi awo akwera mtengo. Mu chikalata chimene bungweli latulutsa, a boma tsopano awapatsa chilolezo choti madzi… ...
Malawi hit with fuel crisis
Mukamva ena akupitirira kunena kuti agona pa filling station chifukwa amasaka mafuta, adziweni ndi opanda chilungamo chabe. Mafuta analonjezedwa kufika lero aja tsopano afika. Ngambwi ngambwi, a Chakwera sakucheza. Patatha sabata a Malawi atazunzika ndi… ...