…Nigerian-Malawian woman married to a Pastor at the centre Details have started emerging of the elaborate doctoral scam that…
…adds Mr Namadingo and Karim in the mix …Nigerian woman attributed with scamming Malawian ‘celebrities’ for 10 million Kwacha per…
Uja amatamika ndi za mafuta ngambwi ngambwi ali kuti? Chifukwa tsopano akuyenera kupepesa a Malawi, azingoyenda ali werawera. Mkulu wa…
Ngati a Peter Mutharika amayesa kuti akadutsa moyela ku convention yawo, apa ndiye aganize kawiri. A Kondwani Nankhumwa sali mocheza…
Mukamva ena akupitirira kunena kuti agona pa filling station chifukwa amasaka mafuta, adziweni ndi opanda chilungamo chabe. Mafuta analonjezedwa kufika…
Mizere yonse mukuyionayi, ati mukuyiona komaliza. Kuyambira lolemba lomweli ili, mafuta akhala paliponse moti malo omwetsera mafuta azichita kuyitanira anthu.…
Olira samugwira pakamwa ndipo mneneri wakale wa chipani chotsutsa cha DPP, a Nicholas Dausi, walira mokweza pa mwambo wa maliro…
…Bullets yakanika kuzemba pa Mazembe Zikakhala nyerere zikuti ndi chifukwa kunalibe ma ref ogulitsa, eni ake a Bullets ati bola…
Kapena mwina a Malawi tasukutsula mmaso pa njuga mpaka takhaulitsa mzungu? Koma a kampani ya Premier Bet ati vuto ndi…
Ati mukamva za anthu osowa, kenako kuzindikira kuti aphedwa, muzingokhala chete basi ndi kumati Chakwera 2025 boma. Ati kufalitsa nkhani…
He is still politicking, even when some families have yet to be found. Even within all this chaos, all he…
Alibe moto Chakwera Mu kufanizira atsogoleri amene Malawi wakhala nawo mu zaka zapitazi, mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera…
Tempers flared in Malawi Parliament this afternoon over the arrest of Anti-Corruption Bureau (ACB) Director, Martha Chizuma, with Parliamentarians exchanging…
As fuel stations run dry in Malawi following a massive economic crisis, people from neighbouring Zambia have also started experiencing…
A majority of respondents in the Afrobarometer survey responded that they would vote back the opposition Democratic Progressive Party (DPP)…