Boma la Malawi lalengeza kuti kuyambira lolemba pa 22 February, masukulu onse atsekulidwa. Izi ndi malingana ndi nduna ya zaumoyo a Khumhize Kandodo Chiponda omweso ndi m’modzi mwa akuluakulu a komiti ya mtsogoleri wa dziko… ...
Articles By Archangel Nzangaya
Malawian concerned students have organized city after city demonstrations starting next week over prolonged school closure due to the COVID-19 pandemic. According to a statement made available to Malawi24, the group through its national chairperson… ...
Apolisi mumzinda wa Lilongwe anjata wachiwiri kwa mkulu wanthambi yowona za ngozi zogwa mwadzidzi a Fyawupi Mwafongo kaamba ka ndalama za mlili wa covid-19. Nkhaniyi ikutsatila kafukufuku yemwe akuchitika zitadziwika kuti ndalama zomwe zimayenera kugwira… ...
Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera achotsa paudindo mkulu wa nthambi yowona za ngozi zogwa mwadzidzi komanso wapampando wa komiti yamtsogoleri wadziko pantchito yothana ndi mlili wa Covid-19 kaamba kakusakazidwa kwa ndalama za Covid-19.… ...
Opposition Democratic Progressive Party (DPP) Spokesperson on Legal Affairs Bright Msaka has told president Lazarus Chakwera to refrain from trying to gag the Malawi Human Rights Commission and Anti-Corruption Bureau (ACB). Msaka was responding to… ...
One of Africa's business tycoons is this year set to launch a digital platform for online shopping and a platform that will connect insurance brokers with clients in Malawi. Announcing the development was Angolan businessperson,… ...
Illovo Sugar Malawi has donated assorted items worth K40 million to Kasinthula COVID-19 Isolation Center in Chikwawa. The company made the donation on Wednesday, February 10, 2021 through the Chikwawa district hospital. The donated items… ...