Malawi24.com
M'modzi mwa madokotala azitsamba odziwika bwino mdziko muno, mai Bwanali am’boma la Neno omwe amadziwika ndi dzina loti Ayaya amwalira. Malingana ndi khansala wa dera la Lisungwi m’boma la Neno a Mark Ngwangwa, mai Bwanali… ...
Pamene anthu ena chimwemwe chinadzadza tsaya kuti nyumba zawo zilumikizidwa magetsi mwaulere, kampani yogulitsa mphamvu za magetsi ya Electricity Supply Corporation of Malawi (ESCOM) yatsutsa malipoti oti yayamba kulumikiza magetsi mwaulere kwa aMalawi. Kumayambiliro kwa… ...