Akatswiri pa ndale ati zomwe achita a chakwera ndi kuphwanya pangano limene anapangana ndi a Malawi kuti iwo ndi nduna zawo sakhalaso ndi ulendo opita kunja kwa dziko lino pokhapokha chuma chitabwezeretsedwa mchimake dziko muno.… ...
Articles By Peter Mavuto
Zatsimikizika kuti mamembala a bhodi ya timu ya mpira wa miyendo ya Mighty Mukuru Wanderers awachotsa. Wapampando wa timuyi a Thomson Mpinganjira atsimikiza za nkhaniyi. Mu chikalata chomwe wasayina ndi mtsogoleriyu chikufotoka kuti izi zadza… ...
Ogwira ntchito mu ma kampani a amwenye mu mzinda wa Blantyre akuti akukakamikizika kuyamba mchitidwe ozembetsa katundu m’malo ogwirira ntchito ndi kumakagulitsa chifukwa cha kuchepa kwa malipiro. M’modzi mwa ogwira ntchito wina yemwe anati tisamutchule… ...
Dziko la Zambia, lomwe ndi neba wa Malawi, lati sukulu ku Zambia zikhalabe zotseka mpaka pa 29 January, 2024 kamba ka muliri wa cholera womwe wabuka m'dzikoli. Chikalata chomwe unduna wa za maphunziro mogwirizana ndi… ...
Pamene madera ambiri dziko lino akhudzidwa ndi vuto losowa mvula yokwanira, pali chiopsezo choti dziko lino likhala lopanda chakudya chokwanira chaka cha mawa. Koma akatswiri pa nkhani za ulimi ati boma likuyenera kulimbikitsa alimi kuti… ...
Akatswiri pa chuma achenjeza anthu m'dziko muno kuti apewe kuononga ndalama mwachisawawa mu nyengo ya khirisimasi komanso mu chikondwerero cha chaka cha tsopano kamba kamavuto a chuma amene ali dziko muno. M'modzi mwa akatswiriwa, a… ...
The Blantyre First Grade Magistrate’s Court on Friday fined Madalisto Kaiwa aged 28 for selling alcohol without a licence at Chilimba Market in Blantyre. Magistrate Soka Banda fined the woman after finding the man guilty… ...