UEFA Champions League (UCL)
Anyamata awiri a timu ya Liverpool Darwin Nunez ndi Curtis Jones ndi omwe anambwandilitsa ma penate awo m'manja mwa goloboyi wa PSG Gianluigi Donnarumma pa bwalo la Anfield usiku wathawu mu mpikisano wa UEFA Champions… ...
Namiwa
Mkulu wa bungwe lomenyera ufulu anthu mdziko muno la Centre for Democracy and Economic Development Initiatives (CDEDI), Sylvester Namiwa wati aMalawi akumanidwa Vitamin A ndi michere ina yomwe imapezeka mu Suga ndipo ndi yofunika kwambiri… ...