![DPP president Peter Mutharika](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2023/12/Peter-Mutharika-DPP-leader-235x176.webp)
Sitinawachotse a Mutharika, latero bungwe la Mulhako
Wapampando wa bhodi ya Mulhako wa Alhomwe watsutsa mphekesera yoti bhodiyi yachotsa mtsogoleri wakale wa dziko lino a Peter Mutharika ngati woyang'anira bungweli. Mukuyankhula kwawo pa msonkhano wa atolankhani mu mzinda wa Blantyre lachiwiri, Muchanakwaye… ...