Mtengo wautali salozerana ndipo nyimbo yomwe yadya nambala one pa YouTube ndi ija ya mkulu odikula uku akutudzula mbina maka ikafika paja akumati "She got me feeling like ah ah ah ah ah ah!" Tsopano… ...
Articles By Ben Bongololo
The Malawi Bureau Standards (MBS) has taken swift action, suspending restaurant operations at Hotel Victoria's and Heritage Hotel by Serindib in Blantyre due to hygiene violations. According to MBS, the immediate suspension of the restaurant… ...
HIV law has remained unknown to many since its introduction in 2018. The National AIDS Commission (NAC) is raising the alarm that a large part of the population is unaware of the HIV and AIDS… ...
Kwachema kwa Manase ku Blantyre pamene apolisi ayamba kunjata anthu onse omwe akugulitsa mowa omwe ndi owopsa ndipo ukutchulidwa ndi mayina monga: Ambuye tengeni, magaga, komanso taya njinga omwe pakadali pano waphapo anthu asanu (5).… ...
Ofesi ya Zaumoyo m'boma la Blantyre yati ikufufuza za imfa ya anthu asanu omwe amwalira kutsatira atamwa mowa osadziwika bwino ndipo ofesiyi yati idzabweretsa poyera zotsatira zakafukufuku-yi akatha. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe khonsolo… ...
Ophunzira wamkazi wa sitandade 5 ku Mulanje wadzipha chifukwa chokwiya ndi malangizo amayi ake omuletsa khalidwe lake lopanga zibwenzi atadziwa kuti akuchita chibwezi ndi m’nyamata wina mdelaro. Nkhani yonse ikuti mtsikanayu, yemwe dzina lake ndi… ...
Kuchema kumabwalo amilandu pomwe bungwe lomwe limathana ndi katangale m'dziko muno la Anti-Corruption Bureau (ACB) lati likuyembekezeka kuzenga milandu khumi, isanu ndi iwiri (17) yokhudza katangale m'mwezi uno wa April ndipo pa milanduyi pali anthu… ...
Boma kudzera muunduna owona za Ulimi m'dziko muno watulutsa mitengo yoyambira kugula mbewu ya chaka chino ndipo mwazina Chimanga chizigulidwa pamtengo wa K650 pa kilogiramu. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe undunawu watulutsa lachinayi pa… ...
Inu anthu omwe mumatuluka kunja kwa dziko lino tamverani! Nthambi ya lmmigration ndi Citizenship Services m'dziko muno yatsutsa mphekesera yoti ziphanso za dziko lino sizikuvomerezedwa pamabwalo ena okwelera ndege. Nthambiyi yanena izi lero kudzera mchikalata… ...
Mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering (ECG), Prophet Shepherd Bushiri, wachenjeza anthu omwe akumema anthu m'masamba amchezo kuti apite munsewu kukachita zionetsero pofuna kukakamiza Mneneriyu kuti apikisane nawo pa udindo wa pulezidenti pa chisankho… ...
Mpungwepungwe unakula m'nyumba ya malamulo pamene mbali ya boma yavomereza lamulo kuti ulimi wachamba udzilimidwa m'dziko muno. Izi zinadzetsa mpungwepungwe kunyumbayi pamene aphungu achipani chotsutsa cha Democratic Progressive Party (DPP) anati sakugwirizana ndi lamuloli. Izi… ...
Anyamata awiri akusungidwa mchitokosi cha apolisi ku Mwanza atagwidwa ndi bomba pa malo ochitira chipikisheni munsewu wa Mwanza-Blantyre pomwe iwo anali pa ulendo wawo okalithira nsika bombali. A Hope Kasakula yemwe ndi wofalitsa nkhani pa… ...
Nduna yoona za chuma mdziko muno a Simplex Chithyola Banda walengeza za kukwera kwa ngongole yomwe ophunzira a msukulu za ukachenjede amalandira kuchoka pa K350, 000 pachaka kufika pa K560,000. A Chithyola Banda anena izi… ...
Mdima wagwanso m'dziko la Nigeria pamene katakwe opanga mafilimu yemwe dzina lake ndi Amaechi Mounagor wadziwika kuti wamwalira atadwala nthenda ya impso. Izi zikudza pasanathe mwezi dzikoli litatayanso katswiri wina a John Okafor yemwe amadziwika… ...
M'modzi mwa anthu omwe amayankhulapo pazochitika m'dziko muno Lyford Chadza wapempha alangizi a mtsogoleri wa dziko lino kuti adzimuwunikira mtsogoleriyu mwatchutchutchu ponena kuti a Chakwera achedwa kulengeza kuti m'dziko muno muli njala. A Chadza ati… ...