![](https://malawi24.com/wp-content/uploads/2019/10/Zomba-prison.jpg)
Mkaidi wathawa ku ndende ya Zomba
Akulu akulu a ndende ya Zomba atsimikiza kuti mkaidi m’modzi wa zaka 33 wathawa pomwe amagwira ntchito lero Lachiwiri. Malinga ndi m’modzi mwa akuluakulu a ndendeyi a Harrings Nyalubwe wazindikira mkaidi othawayu ngati Jimu Jabu.… ...